Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 24:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Pa chifukwa chimenechi, inunso khalani okonzeka,+ chifukwa Mwana wa munthu adzabwera pa ola limene simukuliganizira.

  • Mateyu 25:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Choncho pitirizani kukhala maso+ chifukwa simukudziwa tsiku kapena ola lake.+

  • Chivumbulutso 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho, pitiriza kukumbukira zimene unalandira ndi zimene unamva. Pitiriza kuzitsatira ndipo ulape.+ Ndithudi, ukapanda kudzuka, ndidzabwera ngati wakuba+ ndipo sudzadziwa ngakhale pangʼono ola limene ndidzafike kwa iwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena