Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 25:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Kenako Mfumu idzauza amene ali kudzanja lake lamanja kuti: ‘Bwerani, inu amene mwadalitsidwa ndi Atate wanga. Lowani mu Ufumu umene anakukonzerani kuchokera pachiyambi cha dziko lapansi.*

  • Luka 12:20, 21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma Mulungu anamuuza kuti, ‘Wopanda nzeru iwe, usiku womwe uno moyo wako aufuna. Nanga zinthu zimene wasungazi zidzakhala za ndani?’+ 21 Umu ndi mmene zimakhalira ndi munthu amene wadziunjikira chuma, koma si wolemera kwa Mulungu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena