-
Aroma 2:28, 29Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
28 Amene ali Myuda kunja kokha si Myuda,+ ndiponso mdulidwe wakunja kokha wochitidwa pathupi, si mdulidwe.+ 29 Kukhala Myuda weniweni kuli mumtima+ ndipo mdulidwe wake umakhalanso wamumtima+ wochitidwa ndi mzimu, osati ndi malamulo olembedwa.+ Munthu woteroyo amatamandidwa ndi Mulungu, osati anthu.+
-