Yohane 14:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Sindilankhula nanu zambiri chifukwa wolamulira wa dziko+ akubwera ndipo alibe mphamvu pa ine.+ Machitidwe 14:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Mʼmalo onsewa ankalimbitsa ophunzira+ komanso kuwathandiza kuti apitirize kukhala ndi chikhulupiriro. Ankawauza kuti: “Tiyenera kukumana ndi mavuto ambiri kuti tikalowe mu Ufumu wa Mulungu.”+ 1 Yohane 4:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ana okondedwa, inu ndi ochokera kwa Mulungu, ndipo mwagonjetsa aneneri abodzawo.+ Zili choncho chifukwa amene ali wogwirizana ndi inu+ ndi wamkulu kuposa amene ali wogwirizana ndi dziko.+ 1 Yohane 5:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Aliyense amene ndi mwana wa Mulungu amagonjetsa dziko.+ Ndipo chikhulupiriro chathu chatithandiza kugonjetsa dziko.+ Chivumbulutso 3:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Amene wapambana pankhondo+ ndidzamulola kuti akhale ndi ine pampando wanga wachifumu,+ ngati mmene ine ndinakhalira+ ndi Atate wanga pampando wawo wachifumu nditapambana pankhondo.
22 Mʼmalo onsewa ankalimbitsa ophunzira+ komanso kuwathandiza kuti apitirize kukhala ndi chikhulupiriro. Ankawauza kuti: “Tiyenera kukumana ndi mavuto ambiri kuti tikalowe mu Ufumu wa Mulungu.”+
4 Ana okondedwa, inu ndi ochokera kwa Mulungu, ndipo mwagonjetsa aneneri abodzawo.+ Zili choncho chifukwa amene ali wogwirizana ndi inu+ ndi wamkulu kuposa amene ali wogwirizana ndi dziko.+
4 Aliyense amene ndi mwana wa Mulungu amagonjetsa dziko.+ Ndipo chikhulupiriro chathu chatithandiza kugonjetsa dziko.+
21 Amene wapambana pankhondo+ ndidzamulola kuti akhale ndi ine pampando wanga wachifumu,+ ngati mmene ine ndinakhalira+ ndi Atate wanga pampando wawo wachifumu nditapambana pankhondo.