Mateyu 4:16, 17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 anthu amene ankakhala mumdima anaona kuwala kwakukulu, ndipo anthu amene ankakhala mʼdera lamthunzi wa imfa, kuwala+ kunawaunikira.”+ 17 Kuyambira nthawi imeneyo, Yesu anayamba kulalikira kuti: “Lapani, chifukwa Ufumu wakumwamba wayandikira.”+ Yohane 3:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Kuwala kwafika mʼdziko+ koma mʼmalo mokonda kuwala anthu akukonda mdima popeza ntchito zawo nʼzoipa, nʼchifukwa chake adzaweruzidwe. Yohane 12:46 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 46 Ndabwera monga kuwala mʼdziko,+ kuti aliyense wokhulupirira ine asapitirize kukhala mumdima.+ 1 Yohane 2:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Komabe, ndikukulemberani lamulo latsopano limene Yesu ankalitsatira, limenenso inuyo mukulitsatira, chifukwa mdima ukupita ndipo kuwala kwenikweni kwayamba kale kuunika.+
16 anthu amene ankakhala mumdima anaona kuwala kwakukulu, ndipo anthu amene ankakhala mʼdera lamthunzi wa imfa, kuwala+ kunawaunikira.”+ 17 Kuyambira nthawi imeneyo, Yesu anayamba kulalikira kuti: “Lapani, chifukwa Ufumu wakumwamba wayandikira.”+
19 Kuwala kwafika mʼdziko+ koma mʼmalo mokonda kuwala anthu akukonda mdima popeza ntchito zawo nʼzoipa, nʼchifukwa chake adzaweruzidwe.
8 Komabe, ndikukulemberani lamulo latsopano limene Yesu ankalitsatira, limenenso inuyo mukulitsatira, chifukwa mdima ukupita ndipo kuwala kwenikweni kwayamba kale kuunika.+