Yesaya 53:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Koma Yehova ndi amene anafuna* kuti mtumiki wake aphwanyidwe ndipo anamulola kuti adwale. Ngati mungapereke moyo wake kuti ukhale nsembe yakupalamula,+Iye adzaona ana ake,* adzakhala ndi moyo kwa nthawi yaitali,+Ndipo kudzera mwa iye, zofuna za* Yehova zidzatheka.+ Luka 24:44 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 44 Ndiyeno anawauza kuti: “Pamene ndinali nanu limodzi ndinakuuzani mawu akuti,+ zonse zokhudza ine zimene zinalembedwa mʼChilamulo cha Mose, zimene aneneri analemba komanso zimene zinalembedwa mʼMasalimo ziyenera kukwaniritsidwa.”+ Machitidwe 2:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Munthu ameneyu, amene anaperekedwa mwa kufuna kwa Mulungu+ ndi kudziwiratu kwake zamʼtsogolo, munachititsa kuti aphedwe pokhomeredwa pamtengo ndi anthu osamvera malamulo.+ 1 Petulo 1:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Zoonadi, Mulungu anasankhiratu Khristu anthu asanayambe kuberekana padziko lapansi,+ koma anaonekera pa nthawi yamapeto chifukwa cha inuyo.+
10 Koma Yehova ndi amene anafuna* kuti mtumiki wake aphwanyidwe ndipo anamulola kuti adwale. Ngati mungapereke moyo wake kuti ukhale nsembe yakupalamula,+Iye adzaona ana ake,* adzakhala ndi moyo kwa nthawi yaitali,+Ndipo kudzera mwa iye, zofuna za* Yehova zidzatheka.+
44 Ndiyeno anawauza kuti: “Pamene ndinali nanu limodzi ndinakuuzani mawu akuti,+ zonse zokhudza ine zimene zinalembedwa mʼChilamulo cha Mose, zimene aneneri analemba komanso zimene zinalembedwa mʼMasalimo ziyenera kukwaniritsidwa.”+
23 Munthu ameneyu, amene anaperekedwa mwa kufuna kwa Mulungu+ ndi kudziwiratu kwake zamʼtsogolo, munachititsa kuti aphedwe pokhomeredwa pamtengo ndi anthu osamvera malamulo.+
20 Zoonadi, Mulungu anasankhiratu Khristu anthu asanayambe kuberekana padziko lapansi,+ koma anaonekera pa nthawi yamapeto chifukwa cha inuyo.+