Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 17:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno Yesu anadzudzula chiwandacho ndipo chinatuluka. Nthawi yomweyo mnyamatayo anachira.+

  • Maliko 1:25, 26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma Yesu anadzudzula mzimuwo kuti: “Khala chete, ndipo tuluka mwa iye!” 26 Choncho mzimu wonyansawo unamuchititsa kuti aphuphe ndipo unafuula mokweza. Kenako unatuluka mwa munthuyo.

  • Maliko 1:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Choncho Yesu anachiritsa anthu ambiri amene ankadwala matenda osiyanasiyana+ ndipo anatulutsa ziwanda zambiri. Koma sanalole kuti ziwandazo zilankhule, chifukwa zinkamudziwa kuti ndi Khristu.*

  • Luka 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kenako Yesu anasonkhanitsa atumwi 12 aja nʼkuwapatsa mphamvu ndi ulamuliro pa ziwanda zonse+ komanso kuti azitha kuchiritsa matenda.+

  • Luka 10:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kenako anthu okwana 70 aja anabwerera akusangalala ndipo anauza Yesu kuti: “Ambuye, ngakhale ziwanda zimatigonjera tikagwiritsa ntchito dzina lanu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena