Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 5:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndinu osangalala pamene anthu akukunyozani,+ kukuzunzani komanso kukunamizirani+ zoipa zilizonse chifukwa cha ine.+

  • Machitidwe 16:20, 21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Atafika nawo kwa akuluakulu a zamalamulo, ananena kuti: “Anthu awa akusokoneza kwambiri mzinda wathu,+ komanso iwowa ndi Ayuda. 21 Ndipo akufalitsa miyambo imene kwa ife ndi yosaloleka kuitsatira kapena kuichita, popeza ndife Aroma.”

  • Machitidwe 17:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Atalephera kuwapeza, anakokera Yasoni ndi abale ena kwa olamulira a mzindawo, akufuula kuti: “Anthu awa, amene ayambitsa mavuto kwina konseku, tsopano akupezekanso kuno.+ 7 Ndipo Yasoni wawalandira ngati alendo ake. Anthu onsewa akuchita zotsutsana ndi malamulo a Kaisara. Eti akunena kuti kulinso mfumu ina dzina lake Yesu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena