Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 21:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho iwo anayamba kudandaula motsutsana ndi Mulungu komanso Mose+ kuti: “Nʼchifukwa chiyani munatitulutsa mʼdziko la Iguputo kuti tidzafere mʼchipululu muno? Kuno kulibe chakudya komanso madzi,+ ndipo chakudya chonyansachi chafika potikola.”+ 6 Ndiyeno Yehova anatumiza njoka zapoizoni* pakati pawo, ndipo zinayamba kuwaluma moti Aisiraeli ambiri anafa.+

  • Mateyu 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma Yesu anamuyankha kuti: “Malemba amanenanso kuti: ‘Yehova* Mulungu wanu musamamuyese.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena