Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 11:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma ndikufuna mudziwe kuti mutu wa mwamuna aliyense ndi Khristu.+ Mutu wa mkazi ndi mwamuna+ ndipo mutu wa Khristu ndi Mulungu.+

  • Aefeso 5:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Akazi azigonjera amuna awo+ ngati mmene amagonjerera Ambuye,

  • Akolose 3:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Inu akazi, muzigonjera amuna anu,+ chifukwa zimenezi ndi zoyenera kwa anthu otsatira Ambuye.

  • Tito 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 azikhala oganiza bwino, oyera, ogwira ntchito zapakhomo,* abwino ndiponso ogonjera amuna awo,+ kuti mawu a Mulungu asanyozedwe.

  • 1 Petulo 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mofanana ndi zimenezi, inu akazi muzigonjera amuna anu+ kuti ngati safuna kumvera Mawu a Mulungu, akopeke ndi khalidwe lanu, osati ndi mawu anu+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena