Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 14:34, 35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 akazi azikhala chete mʼmipingo, chifukwa nʼzosaloleka kuti iwo azilankhula,+ koma azigonjera,+ ngati mmenenso Chilamulo chimanenera. 35 Ngati akufuna kumvetsa zinazake, akafunse amuna awo kunyumba, popeza nʼzochititsa manyazi kuti mkazi azilankhula mumpingo.

  • 1 Petulo 3:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mofanana ndi zimenezi, inu akazi muzigonjera amuna anu+ kuti ngati safuna kumvera Mawu a Mulungu, akopeke ndi khalidwe lanu, osati ndi mawu anu+ 2 koma chifukwa choti aona khalidwe lanu labwino*+ komanso ulemu wanu waukulu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena