Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 22:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mphamvu zanga zauma ngati phale.+

      Lilime langa lamatirira kunkhama zanga,+

      Ndipo mwandilowetsa mʼdzenje kuti ndife.+

  • Yesaya 53:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye anaponderezedwa ndipo anatengedwa popanda kuweruzidwa mwachilungamo.

      Ndi ndani amene anaganizira tsatanetsatane wa mʼbadwo wa makolo ake?*

      Popeza iye anadulidwa mʼdziko la anthu amoyo.+

      Iye anakwapulidwa* chifukwa cha zolakwa za anthu anga.+

  • Yesaya 53:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa chifukwa chimenechi, ndidzamupatsa gawo pamodzi ndi ambiri,

      Ndipo iye adzagawana ndi amphamvu katundu amene alanda kunkhondo,

      Chifukwa anapereka moyo wake*+

      Ndipo anaikidwa mʼgulu la anthu ochimwa.+

      Ananyamula tchimo la anthu ambiri+

      Ndipo analowererapo kuti athandize anthu ochimwa.+

  • Danieli 9:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pambuyo pa milungu 62 imeneyi, Mesiya adzaphedwa+ ndipo sadzasiya kalikonse.+

      Mtsogoleri adzabwera ndi gulu lake lankhondo ndipo adzawononga mzindawo ndi malo oyera.+ Malo oyerawo adzafafanizidwa ndi madzi osefukira ndipo padzakhala nkhondo mpaka kumapeto. Mogwirizana ndi zimene Mulungu wasankha, kudzakhala chiwonongeko.+

  • 1 Petulo 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Iye ananyamula machimo athu+ mʼthupi lake pamene anamukhomerera pamtengo.+ Anachita zimenezi kuti tipulumutsidwe ku uchimo nʼkumachita zinthu zolungama. Ndipo “munachiritsidwa ndi mabala ake.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena