Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 16:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Yesu anamuuza kuti: “Ndiwe wosangalala Simoni mwana wa Yona, chifukwa si munthu* amene wakuululira zimenezi, koma Atate wanga amene ali kumwamba ndi amene wachita zimenezi.+

  • Maliko 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iye anawauza kuti: “Inu mwapatsidwa mwayi woti mumvetse chinsinsi chopatulika+ cha Ufumu wa Mulungu. Koma amene ali kunja amauzidwa zonse pogwiritsa ntchito mafanizo+

  • Aefeso 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mʼmibadwo yamʼmbuyo, chinsinsi chimenechi sichinaululidwe kwa ana a anthu mmene Mulungu wachiululira panopa kwa atumwi ndi aneneri ake oyera kudzera mwa mzimu.+

  • 2 Timoteyo 1:9, 10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Iye anatipulumutsa ndiponso anatiitana kuti tikhale oyera,+ osati chifukwa cha ntchito zathu, koma chifukwa cha cholinga chake ndi kukoma mtima kwake kwakukulu.+ Mulungu anatisonyeza kukoma mtimaku kalekale chifukwa cha Khristu Yesu. 10 Koma tsopano izi zatsimikizirika chifukwa cha kuonekera kwa Mpulumutsi wathu Khristu Yesu,+ amene wathetsa mphamvu za imfa.+ Komanso pogwiritsa ntchito uthenga wabwino,+ watidziwitsa mmene tingapezere moyo+ wosawonongeka.+

  • 1 Petulo 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mulungu anauza aneneriwo kuti sankadzitumikira okha, koma ankatumikira inuyo. Tsopano zinthu zimenezi zaululidwa ndi anthu omwe akulengeza uthenga wabwino kwa inu mothandizidwa ndi mzimu woyera wochokera kumwamba.+ Angelo amafunitsitsa atamvetsa zinthu zimenezi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena