Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 52:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chokanimo, chokanimo, tulukani mmenemo,+ musakhudze chinthu chilichonse chodetsedwa!+

      Chokani pakati pake!+ Khalani oyera,

      Inu amene mukunyamula ziwiya za Yehova.+

  • Yeremiya 51:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 45 Tulukani mʼBabulo anthu anga.+

      Thawani mkwiyo wa Yehova+ woyaka moto kuti mupulumutse moyo wanu.+

  • Chivumbulutso 18:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndinamva mawu ena kuchokera kumwamba akuti: “Tulukani mwa iye anthu anga,+ ngati simukufuna kugawana naye machimo ake ndiponso ngati simukufuna kulandira nawo ina ya miliri yake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena