Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 19:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Usabwezere choipa+ kapena kusungira chakukhosi anthu a mtundu wako. Uzikonda mnzako mmene umadzikondera wekha.+ Ine ndine Yehova.

  • Mateyu 7:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Choncho zinthu zonse zimene mukufuna kuti anthu akuchitireni, inunso muwachitire zomwezo.+ Zimenezi ndi zomwe Chilamulo chimafuna komanso zimene aneneri analemba.+

  • Mateyu 22:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Lachiwiri lofanana nalo ndi ili: ‘Uzikonda mnzako mmene umadzikondera wekha.’+

  • Aroma 13:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Anthu inu musamakhale ndi ngongole iliyonse kwa munthu aliyense, kupatulapo kukondana,+ popeza amene amakonda munthu mnzake wakwaniritsa lamulo.+ 9 Chifukwa malamulo onena kuti, “usachite chigololo,+ usaphe munthu,+ usabe,+ usasirire mwansanje,”+ ndiponso lamulo lina lililonse limene lilipo, chidule chake chili mʼmawu awa akuti: “Uzikonda mnzako mmene umadzikondera wekha.”+

  • Yakobo 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiye ngati mukutsatira lamulo lachifumu lakuti, “Uzikonda mnzako mmene umadzikondera wekha,”+ ngati mmene lemba limanenera, mukuchita bwino ndithu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena