Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 6:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Mosiyana ndi zimenezo, inu pitirizani kukonda adani anu. Pitirizani kuchita zabwino ndi kukongoza popanda chiwongoladzanja, osayembekezera kulandira kalikonse.+ Mukatero, mphoto yanu idzakhala yaikulu ndipo mudzakhala ana a Wamʼmwambamwamba, chifukwa iye ndi wokoma mtima kwa osayamika ndi kwa oipa.+

  • Aroma 2:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kodi sukudziwa kuti Mulungu akukusonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu,+ kusakwiya msanga+ komanso kuleza mtima+ nʼcholinga choti ulape?+

  • Aefeso 4:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Koma muzikomerana mtima, muzisonyezana chifundo chachikulu+ komanso muzikhululukirana ndi mtima wonse, ngati mmene inunso Mulungu anakukhululukirani ndi mtima wonse kudzera mwa Khristu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena