-
Akolose 2:16, 17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Choncho musalole kuti munthu aliyense akuweruzeni chifukwa cha chakudya ndi chakumwa+ kapena chikondwerero chinachake kapenanso kusunga tsiku limene mwezi watsopano waoneka+ kapena kusunga sabata.+ 17 Zinthu zimenezi ndi mthunzi wa zimene zinali kubwera,+ koma zenizeni zake zinakwaniritsidwa ndi Khristu.+
-