Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Akorinto 13:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pomaliza abale, pitirizani kusangalala, kusintha maganizo, kulimbikitsidwa,+ kukhala ndi maganizo ogwirizana+ ndiponso kukhala mwamtendere.+ Mukatero, Mulungu amene ndi wachikondi komanso wamtendere+ adzakhala nanu.

  • 1 Atesalonika 5:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Muziwasonyeza chikondi komanso ulemu waukulu chifukwa cha ntchito yawo.+ Muzikhala mwamtendere pakati panu.+

  • 2 Petulo 3:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho okondedwa, popeza mukuyembekezera zinthu zimenezi, yesetsani kuchita zonse zimene mungathe kuti Mulungu adzakupezeni muli oyera, opanda cholakwa ndiponso muli mumtendere.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena