2 Mbiri 19:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Ndiyeno Yehu+ mwana wa Haneni+ wamasomphenya, anapita kwa Mfumu Yehosafati ndipo anamufunsa kuti: “Kodi muyenera kuthandiza anthu oipa,+ ndipo kodi muyenera kukonda anthu odana ndi Yehova?+ Chifukwa cha zimenezi Yehova wakukwiyirani. Yohane 15:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Mukanakhala mbali ya dziko, dziko likanakukondani monga mbali yake. Popeza simuli mbali ya dzikoli,+ koma ine ndinakusankhani kuchokera mʼdziko, pa chifukwa chimenechi dziko likudana nanu.+ Yohane 17:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Iwo ndawapatsa mawu anu, koma dziko likudana nawo chifukwa sali mbali ya dziko,+ mofanana ndi ine amene sindili mbali ya dziko. Yohane 18:36 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 Yesu anayankha kuti:+ “Ufumu wanga si wamʼdzikoli.+ Ufumu wanga ukanakhala wamʼdzikoli, atumiki anga akanamenya nkhondo kuti ndisaperekedwe kwa Ayuda.+ Koma Ufumu wanga si wochokera mʼdzikoli.” 1 Yohane 2:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Musamakonde dziko kapena zinthu zamʼdziko.+ Ngati wina akukonda dziko, ndiye kuti sakonda Atate.+ 1 Yohane 5:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Tikudziwa kuti ndife anthu a Mulungu, koma dziko lonse lili mʼmanja mwa woipayo.*+
2 Ndiyeno Yehu+ mwana wa Haneni+ wamasomphenya, anapita kwa Mfumu Yehosafati ndipo anamufunsa kuti: “Kodi muyenera kuthandiza anthu oipa,+ ndipo kodi muyenera kukonda anthu odana ndi Yehova?+ Chifukwa cha zimenezi Yehova wakukwiyirani.
19 Mukanakhala mbali ya dziko, dziko likanakukondani monga mbali yake. Popeza simuli mbali ya dzikoli,+ koma ine ndinakusankhani kuchokera mʼdziko, pa chifukwa chimenechi dziko likudana nanu.+
14 Iwo ndawapatsa mawu anu, koma dziko likudana nawo chifukwa sali mbali ya dziko,+ mofanana ndi ine amene sindili mbali ya dziko.
36 Yesu anayankha kuti:+ “Ufumu wanga si wamʼdzikoli.+ Ufumu wanga ukanakhala wamʼdzikoli, atumiki anga akanamenya nkhondo kuti ndisaperekedwe kwa Ayuda.+ Koma Ufumu wanga si wochokera mʼdzikoli.”