Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g87 12/8 tsamba 32
  • Zisonyezero za Voliyamu 31 ya “Galamukani!”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Voliyamu 31 ya “Galamukani!”
  • Galamukani!—1987
  • Timitu
  • ACHICHEPERE AKUFUNSA KUTI . . .
  • CHIPEMBEDZO
  • UMOYO NDI MANKHWALA
  • CHUMA NDI NTCHITO YOLEMBEDWA
  • LINGALIRO LABAIBULO
  • MAIKO NDI ANTHU
  • MAUNANSI A ANTHU
  • MBONI ZA YEHOVA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • NYAMA NDI ZOMERA
  • SAYANSI
  • ZOCHITIKA ZADZIKO NDI MIKHALIDWE
Galamukani!—1987
g87 12/8 tsamba 32

Zisonyezero za Voliyamu 31 ya “Galamukani!”

ACHICHEPERE AKUFUNSA KUTI . . .

Kodi Baibulo Nloyenerera kwa Ine? 2/8

Kodi Cholakwika Nchiyani ndi Kukhala ndi Nthaŵi Yabwino? 4/8

Kodi Cholakwika Nchiyani ndi Kulimba Mtima? 2/8

Kodi Kuseka Kogwira Ntchito Sikuli Chabe Chiphwete Chosavulaza? 7/8

Kodi Nchifukwa Ninji Achikulire Samandimvetsetsa? 4/8

Kodi Nchifukwa Ninji Amayi Samapezeka Pamene Ndifika Panyumba? 3/8

Kodi Ndimotani Mmene Ndingachirire ku Kugwiritsira Ntchito Molakwa Mankhwala Ogodomalitsa? 5/8

Kodi Ndimotani Mmene Ndingathandizire Achikulire Kundimvetsetsa? 5/8

Kodi Ndingalamulire Motani Kupsya Mtima Kwanga? 10/8

Kodi Ndingalimbane Ndi Kupsyinjika? 8/8

Kodi Ndingapeze Bwanji Chisangalalo Monga Mwana Yekha? 11/8

Kodi Ndingaphunzire Motani Pamene Mphunzitsi Wanga Ali Wogwetsa Ulesi Chotero? 1/8

Kodi Ndiyenera Kutsatira Machitachita Aposachedwapa? 6/8

Kodi Sitingathe Kukhala Mabwenzi Chabe? 1/8

Makolo Anga Amagwira Ntchito—Kodi Ndingachitenji Ndekha M’nyumba Yopanda Kanthu? 6/8

Nchifukwa Ninji Ndimapsya Mtima? 9/8

Nchiyani Chimandipangitsa Kudzimva Wosungulumwa Chotero? 12/8

CHIPEMBEDZO

Baibulo Kodi Kapena Mwambo?—Chothetsa Nzeru kwa Akatolika Owona Mtima 3/8

Chigumula Ndi Chirala—Kodi Ndizochita za Mulungu? 3/8

Chipembedzo mu Ndale Zadziko—Kodi Ichi Chiri Chifuno cha Mulungu? 9/8

Chowonadi Ponena za Miyambo ya Isitala 4/8

Kodi Matsoka ali “Zochita za Mulungu?” 6/8

Kukhulupirika kwa Masiku a Baibulo Nkosatsutsika 7/8

‘Manja Anu Adzaza ndi Mwazi’ 12/8

Mawonekedwe Osiyanasiyana a Isitala 3/8

‘Mwenzi Onse Atakhala Aneneri!’ 3/8

Nchifukwa Ninji Atsogoleri Achipembedzo Amasanganizira mu Ndale Zadziko? 9/8

Nsanja ya Babele Yamakono? 12/8

Silirinso Bukhu Loletsedwa 3/8

UMOYO NDI MANKHWALA

AIDS, Kuthiriridwa Mwazi, ndi Mboni za Yehova 1/8

Bwanji Ponena za Umoyo Wabwino wa Inu Eni? 10/8

Kensa—Kodi Tikuchita Motani? 4/8

“Kensa—Ndikuigonjetsa” 4/8

Kodi Mungagonjetse Kensa? Kodi Choichititsa Nchiyani? 4/8

Kodi Mungagonjetse Kensa? 4/8

Kuchiritsa Kosatha Kuli Pafupi 10/8

Kuchotsa Mimba—Chidziŵitso Chidzetsa Thayo 8/8

Kuchotsa Mimba—Dziko Logawanika 8/8

Kuchotsa Mimba—Kodi Ndani ali Wokhoza? 8/8

Kuchotsa Mimba—Ndi Magwero a Moyo 8/8

Kuchotsa Mimba—Pa Mtengo Wapatali 8/8

Kudwala Maganizo—Kodi Pali Kuchiritsa Kuli Konse? 7/8

Kudwala Maganizo—Nthenda ya Chinsinsi 7/8

Kusakaza Kokulira kwa Fodya mu Greece 10/8

“Ngwazi ya Nkhokera” 10/8

Pamene Kensa Idzaleka 4/8

Sammy Wamng’onoyo Anaphedwa ndi AIDS! 2/8

Thanzi Labwino M’chikho cha Madzi! 1/8

CHUMA NDI NTCHITO YOLEMBEDWA

Akazi Ogwira Ntchito—Mmene Maiko Osatukuka Amawonera 2/8

LINGALIRO LABAIBULO

Kodi Helo Ngwotentha? 6/8

Kodi Kukhulupirira Malaulo Kuli Kosavulaza? 10/8

Kodi Mulungu Anali ndi Chiyambi? 2/8

Kulankhula M’malirime—Kodi Nkochokera kwa Mulungu? 8/8

Ndani Angatonthoze ‘Kulira kwa Njala’? 12/8

MAIKO NDI ANTHU

Akasupe a Moto ku Hawaii 10/8

Chipwirikiti mu South Africa 4/8

Dziko Losagwirizana—Kodi Chothetsera Nchiyani? 4/8

Kodi Kunayambira Kuti? 8/8

Mtendere, Chigwirizano, ndi Chikondi Pakati pa Kusakhazikika kwa Zinthu 3/8

MAUNANSI A ANTHU

Bongo Wodabwitsa Umenewu wa Khanda 11/8

Chisonkhezero Kaamba ka Mphamvu za Nzeru Zozizwitsa 11/8

Kodi Nkukwatiriranji? 5/8

Kuchokera ku Chikuta Kufika ku Manda—Chosowa Chathu Chachikulu Ndi Chikondi 7/8

Kukhalira Limodzi Kapena Ukwati? 5/8

Machitachita Owonjezereka ku Ukwati—Kulekeranji? 5/8

Njira ya Moyo ya Ogonana Ofanana Ziwalo—Kodi Iri Yamoyo Kwambiri Motani? 1/8

Phunzitsani Mwana Wanu m’Njira Yabwino—Ndipo Kuchiteni Kuchokera ku Ukhanda! 11/8

Ukwati—Ngwoyenerera? 5/8

Umoyo Wabwino Kaamba ka Mtundu Wonse wa Anthu—Liti? 10/8

MBONI ZA YEHOVA

Chitonthozo kwa Wolapa 6/8

“Kulankhula za Kugwirira Ntchito Pamodzi” 8/8

Kupeza Gulu la Nkhondo Labwino 9/8

Ndinamva Dzina la Mulungu ndi Kuiwala la Mwinine 5/8

Ndiri Woyamikira ndi Zimene Ndiri Nazo 10/8

Ntchito ya Magazini ku Japan Ibwera ‘Mu Dongosolo’ 9/8

Omaliza Maphunziro a Gileadi Akudziika Pansi pa Chitsogozo cha Mulungu 3/8

Trinidad Akuimanga m’Masiku Anayi! 1/8

“Tsopano Udzafa!” 1/8

Ziŵanda Zindiposa Mphamvu 6/8

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Allan Kardec—Ngwazi ya Kukhulupirira Mizimu 11/8

Kodi Chothetsera Nchiyani? 3/8

Kodi Mungatseke Danga la Mbadwo? 5/8

Kupambutsira Ndege ku Malta—Koma Ndinapulumuka 3/8

Kupenda Nyenyezi—Kodi Ndimaseŵera Osavulaza? 2/8

Kupenda Nyenyezi Kuyambanso! 2/8

Mbala Yosankha 3/8

Mtsogolo Mwanu—Kodi Munalembedwa m’Nyenyezi? 2/8

NYAMA NDI ZOMERA

Katungulume—Zipatso Zonga Ntedza 9/8

Khalani ndi Moyo Kuti Mudzawone Nkhalango Zikusangalala 12/8

Kodi Nkhalango Zingasungidwe? 12/8

Kumanani ndi Kasenye Kakang’ono Koposa m’Dziko 10/8

Mvula ya m’Nyengo Yachisanu Imabweretsa Maluŵa a m’Chipululu—Ndiponso Zosungira za Zomera Zomadzazanso 11/8

“Ndidyeni Ngati Mulibe Mantha” 11/8

SAYANSI

Koloko ya Radiocarbon 7/8

Kulankhula ndi Kupenya Kupyolera m’Galasi 11/8

Masiku a Usayansi a Nthaŵi Zakale 7/8

Maso m’Mlengalenga 9/8

ZOCHITIKA ZADZIKO NDI MIKHALIDWE

Bombalo ndi Mtsogolo mwa Munthu 2/8

Chida Chankhondo Chotsirizira ndi Kulimbanira Chisungiko 2/8

Chigwirizano cha Mitundu Chidzandira ku Imfa Yake 10/8

Chigwirizano cha Mitundu, Chosonkhezeredwa ndi Mantha 11/8

‘Kamodzi Koyambira Ulendo’ 1/8

Kodi Nchiyani Chachitika ku Nthaka Yathu? 7/8

Kufunafuna Chisungiko m’Mbadwo wa Bomba 2/8

Kumwa ndi Kuyendetsa Galimoto—Kodi Nchiyani Chimene Chingachitidwe? 1/8

Kupsyinjika kwa Dziko Lapansi Ndipo ku Nkhondo Kachiŵirinso 9/8

Maseŵera a Chihuligani—Kodi Ndi Nthenda Kapena Chizindikiro? 1/8

Nkhondo ya Dziko II—Kutha Kwake Kowopsya ndi Kwamoto 12/8

Uchigawenga—Kodi Aliyense Ngwotetezereka? 3/8

Zaka za m’Makumi Aŵiri Zobangula—Zikhala Bata Pamaso pa Namondwe 8/8

Zoledzeretsa ndi Inu 1/8

Zoledzeretsa ndi Kuyendetsa Galimoto 1/8

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena