Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g89 12/8 tsamba 32
  • Zisonyezero za Volyumu 33 ya Galamukani!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Volyumu 33 ya Galamukani!
  • Galamukani!—1989
  • Timitu
  • ACHICHEPERE AKUFUNSA KUTI . . .
  • CHIPEMBEDZO
  • CHUMA NDI NTCHITO YOLEMBEDWA
  • LINGALIRO LABAIBULO
  • MAIKO NDI ANTHU
  • MBONI ZA YEHOVA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • NYAMA NDI ZOMERA
  • SAYANSI
  • UMOYO NDI MANKHWALA
  • ZOCHITIKA ZADZIKO NDI MIKHALIDWE
Galamukani!—1989
g89 12/8 tsamba 32

Zisonyezero za Volyumu 33 ya Galamukani!

ACHICHEPERE AKUFUNSA KUTI . . .

Kodi Angachitirenji Motero kwa Ine? 11/8

Kujeda, 7/8, 8/8

Kukambitsirana, 6/8

Kukhalabe Mabwenzi, 10/8

Kukhala Chitsanzo kwa Achichepere? 11/8

Kumenyana kwa Makolo, 12/8

Kunyada kwa Ufuko, 2/8

Kupalana Ubwenzi Kwachipambano, 3/8, 5/8

Kusamalira Ndalama Zanga, 1/8

Kusankha Zovala, 10/8

Kutukwana, 9/8

Ntchito, 2/8

Nyimbo Zachikondi, 7/8

Ovutitsa Kusukulu, 8/8

Wokonzekera Kuyendetsa? 3/8, 4/8

CHIPEMBEDZO

Bwalo Lankhondo la Milungu, 2/8

Chihindu—Dzina Lanu Liri Kulekerera, 4/8

Chipembedzo Chofunikira Kukonzanso, 9/8

Chipembedzo—Chonyenga Cholakidwa ndi Nthaŵi Yake Yapita! 12/8

Chiprotesitanti—Kodi Chinali Kukonzanso? 9/8

Chiwunikiro Chomwe Chinalonjeza Ufulu (Chibuda), 5/8

‘Choloŵetsedwa m’Kugwa Kokulira Kwa Makhalidwe Abwino,’ 1/8

Dziko Lachikristu Lilimbana ndi Kusintha Kwadziko, 10/8

Kodi Apapa Samalakwa? 2/8

Kubwezeretsedwa Kuyandika! 11/8

Kuchokera Mu Mdima, Chinachake “Choyera,” 7/8

Kuchotsa Kuunika kwa Uthenga Wabwino, 7/8

Kudikirirabe Mesiya, 6/8

Kufufuza kwa Kum’mawa kaamba ka Njira Yolondola, 4/8

Kugonjera ku Chifuniro cha Mulungu (Chisilamu), 8/8

Kusagwirizana Kwa Chipembedzo—Mmene Kunayambira, 1/8

Kutembenukira ku Lupanga, 8/8

Kuyang’ana Kosamalitsa pa Chipembedzo, 1/8

Milungu ya Nthanthi Yopanda Phindu, 3/8

Mpalu, Nsanja, ndi Inu! 2/8

Mtundu Woikidwa Pambali (Israyeli), 3/8

Njira ya Chikhulupiriro, Chiyembekezo, ndi Chikondi (Chikristu), 6/8

Njira Zopeŵera Kutenga Mimba—Kodi Ndani Ayenera Kusankha? 10/8

Nthaŵi Yoŵerengera Yayandikira, 12/8

Pamene “Akristu” ndi “Akunja” Anakumana, 10/8

Zogulidwa Kwambiri za Chipembedzo (Mabukhu Opatulika), 4/8

Zovala Zokhathamira ndi Mwazi, 11/8

Zozizwitsa ndi Masomphenya, 3/8

CHUMA NDI NTCHITO YOLEMBEDWA

Kubwezeretsa Chuma, 5/8

Vuto la Mtengo wa Kakhalidwe, 5/8

LINGALIRO LABAIBULO

Kodi Kulambira Makolo Kuli Kwachikristu? 3/8

Kodi Muyenera Kuwopa Diso Lankhwezule? 2/8

Kodi Wochita Kugonana kwa Ofanana Ziŵalo Angakhale Mtumiki wa Mulungu? 8/8

Kugonana kwa Ofanana Ziŵalo—Kodi Nchiyani Chimene Chiri Thayo la Atsogoleri Achipembedzo? 9/8

Kugonana kwa Ofanana Ziwalo—Nkulekeranji? 7/8

Kusuta—Maupanduwo, 11/8

Nchiyani Chomwe Chiri Chifuno cha Moyo? 2/8

MAIKO NDI ANTHU

Kuthetsa Mavuto a Osauka, 1/8

Tchalitchi m’Ndale Zadziko (Brazil), 1/8

MBONI ZA YEHOVA

Kuchilikizidwa ndi Chiyembekezo cha Ufumu, 11/8

Kuchokera ku Mpandu Kukhala Mkristu, 10/8

Nthanthi Yonena Zaumulungu Siiri Kaamba ka Ine (A. Monteiro Carneiro), 1/8

“Sitipatsa Mlandu Mulungu,” 8/8

Sitolo Yochedwetsedwa, 8/8

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Kugwirira Chigololo—Anachinjirizidwa ndi Zimene Anaŵerenga, 9/8

Kukongola kwa Mkati (Geode), 2/8

“Mfungulo ku Ngozi” (Mfuti), 6/8

Miyambo ya Krisimasi, 12/8

Zimene Mwana Wosabadwa Amadziŵa, 11/8

NYAMA NDI ZOMERA

“Imodzi ya Ntchito Zaluso Zachibadwa” (Njovu), 3/8

SAYANSI

“Chilengedwe cha Ponseponse Chonse Mkati mwa Chigaza,” 2/8

Yochepera koma Yokhala ndi Zitsogozo Zapadera (DNA), 8/8

UMOYO NDI MANKHWALA

Kodi Kutaya Kulemera Kuli Nkhondo Yosagonjetseka? 6/8

Kusuta, 7/8, 8/8

Mwazi: Chosankha Chandani ndi Chikumbumtima Chandani? 3/8

Njira Zinayi Zopambanira, 6/8

Nsabwe za M’mutu, 9/8

Thandizo kwa Okhala ndi Zosoŵa Zapadera (Kulemala Kwa Nzeru Zodziŵira Zinthu), 8/8

Umoyo Wabwino, 12/8

ZOCHITIKA ZADZIKO NDI MIKHALIDWE

Chipululutso, 4/8

Chiwawa—Kodi Tikuchifikira Chitokoso? 5/8

Chiwawa—Mapeto Akuwonekera, 5/8

Dziko Lopanda Zida, 6/8

Kodi Nchiyani Chikuchitika ku Makhalidwe? 8/8

Kodi Nchiyani Chimene Chikuchitika ku Maseŵera? 11/8

Kufunafuna Mtendere ndi Chisungiko, 12/8

Kuyendayenda mu Imfa (Zida Zankhondo), 6/8

Malonda a Zida Zankhondo, 6/8

Nkhondo—Kuchita ndi Zotulukapo Zake, 10/8

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena