Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g91 11/8 tsamba 32
  • Makope 15,290,000 A Kope Lirilonse m’Zinenero 110

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Makope 15,290,000 A Kope Lirilonse m’Zinenero 110
  • Galamukani!—1991
Galamukani!—1991
g91 11/8 tsamba 32

Makope 15,290,000 A Kope Lirilonse m’Zinenero 110

Nsanja ya Olonda iri mosayerekezeka magazini achipembedzo ofalitsidwa koposa padziko lonse. Kunena zowona, ali magazini ochepekera amtundu wake amene aposa kufalitsidwa kwake. Kodi nchifukwa ninji imaŵerengedwa mofala chotero?

Imalongosola mmene dziko latsopano lolungama posachedwapa lidzakhazikitsidwira, ikumapatsa oŵerenga ake chiyembekedzo chotsimikizirika ndipo chowona kaamba ka mtsogolo. Kodi mungakonde kuti Nsanja ya Olonda itumizidwe kunyumba kwanu? Ngati kuli choncho, chonde dzazani ndi kutumiza katikiti kotsatiraka.

Ndingakonde kuti magazini a Nsanja ya Olonda atumizidwe kunyumba kwanga. (Kunja kwa Zambia, lemberani nthambi ya Watch Tower yakwanuko kaamba ka chidziŵitso. Onani tsamba 5.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena