Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g91 11/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1991
  • Timitu
  • Kuwonjezereka Kwakukulu kwa Anthu—Kodi Kumawopseza Mtsogolo Mwathu? 3-14
  • Kodi Kutchova Juga Kulidi Koipa Kwambiri? 19
Galamukani!—1991
g91 11/8 tsamba 2

Tsamba 2

Kuwonjezereka Kwakukulu kwa Anthu—Kodi Kumawopseza Mtsogolo Mwathu? 3-14

“Kuwonjezereka kwakukulu kwa anthu,” “ngozi ya kuchuluka kwa anthu,” “kupanikiza kwa chiphunzitso cha Malthus”—ameneŵa ndiochepa chabe a mawu ogwiritsiridwa ntchito kufotokoza chiwopsezo cha mkhalidwe wa moyo wamtsogolo. Koma kodi bwanji ponena za tsopano lino? Kodi kuwonjezereka kwakukulu kwa anthu kungakuyambukireni motani? Kodi ndimotani mmene kuliri kukhala ndi moyo m’mizinda mmene anthu amakhala mopanikizana kwambiri? Ndipo bwanji ponena za mtsogolo? Mpambo uno wa nkhani ukupenda mafunso ameneŵa.

Kodi Kutchova Juga Kulidi Koipa Kwambiri? 19

Ambiri amamwerekera ndi kutchova juga adakali achichepere. Kodi kungatsogolere kuchiyani? Kodi nchifukwa ninji muyenera kukaniza chisonkhezerocho?

 

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena