Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g92 5/8 tsamba 2
  • Tsamba 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 2
  • Galamukani!—1992
  • Timitu
  • Thandizani! Ndife Alendo 3-12
  • Kodi Nchifukwa Ninji Ndiyenera Kufika Msanga Panyumba? 28
Galamukani!—1992
g92 5/8 tsamba 2

Tsamba 2

Thandizani! Ndife Alendo 3-12

Pafupifupi dziko lirilonse liri ndi alendo—anthu mamiliyoni ambiri osamuka kwawo. Angakhale akugwira ntchito pamodzi nanu kapena kusamukira kwanuko. Mwatsoka lanji, amawonedwa kaŵirikaŵiri kukhala chiwopsezo. Koma nkhani iriyonse imakhala ndi mbali ziŵiri nthaŵi zonse. Chotero, kodi nchifukwa ninji amasamuka? Kodi alidi chiwopsezo? Kodi nchiyani chomwe mungachite kuwathandiza?

Kodi Nchifukwa Ninji Ndiyenera Kufika Msanga Panyumba? 28

Mwachiwonekere achichepere akufunsa funso limeneli padziko lonse. Chotero nchifukwa ninji makolo amakhazikitsira ana awo nthaŵi yausiku yoyenera kufika panyumba?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena