Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g98 4/8 tsamba 32
  • April 11, 1998—Tsiku Loyenera Kukumbukira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • April 11, 1998—Tsiku Loyenera Kukumbukira
  • Galamukani!—1998
Galamukani!—1998
g98 4/8 tsamba 32

April 11, 1998—Tsiku Loyenera Kukumbukira

Usikuwo asanafe, Yesu anapatsa atumwi ake mkate wopanda chotupitsa ndi chikho cha vinyo ndipo anawauza kuti adye ndi kumwa. Komanso anawauza kuti: “Chitani ichi chikumbukiro changa.”—Luka 22:19.

Chaka chino kukumbukira zimenezi kudzakhalako Loŵeruka pa April 11, dzuŵa litaloŵa. Mboni za Yehova kuzungulira dziko lonse lapansi zidzasonkhana usiku wapadera umenewu kudzachita Chikumbutso monga mmene Yesu analamulirira. Tikukuitanani kuti mudzakhale nafe kuti mudzaonerere. Chonde funsani Mboni za Yehova zakwanuko za nthaŵi yeniyeni ndi malo kumene kudzakhale msonkhano.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena