Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g99 12/8 tsamba 31
  • Zisonyezero za Voliyumu 80 ya Galamukani!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Voliyumu 80 ya Galamukani!
  • Galamukani!—1999
  • Timitu
  • ACHINYAMATA AKUFUNSA
  • CHIPEMBEDZO
  • CHUMA NDI NTCHITO
  • LINGALIRO LA BAIBULO
  • MAUNANSI A ANTHU
  • MAYIKO NDI ANTHU
  • MBONI ZA YEHOVA
  • NKHANI ZA MOYO WA ANTHU
  • UMOYO NDI MANKHWALA
  • ZINYAMA NDI ZOMERA
  • ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MIKHALIDWE YAKE
  • ZOSIYANASIYANA
Galamukani!—1999
g99 12/8 tsamba 31

Zisonyezero za Voliyumu 80 ya Galamukani!

ACHINYAMATA AKUFUNSA

Chibwenzi ndi Munthu Amene Akukhala Kutali, 2/8

Kukhala Wochezeka? 11/8, 12/8

Kupirira Kusoŵa Chilungamo? 10/8

Kutonzedwa, 7/8

Maseŵero Odziyerekeza Kukhala Munthu Wotchuka, 9/8

Miseche, 3/8

N’chifukwa Chiyani Amayi Anga Akudwala Chomwechi? 8/8

N’chifukwa Chiyani Ndimaopa Kunenepa? 5/8

N’chifukwa Chiyani Sindikutha Kupeza Zinthu Zimene Ndimafuna? 4/8

Ndingakhale Motani Wopanda Makolo? 1/8

Vuto Loopa Kunenepa, 6/8

CHIPEMBEDZO

Kodi Mukufuna Kukondweretsa Mulungu? 1/8

Kodi Mulungu Alikodi? 2/8

Kukambirana za Chipembedzo, 3/8

N’chikonzero cha Mulungu? 8/8

Ufulu Wachipembedzo Ukuponderezedwa, 1/8

Wosakhulupirira Mulungu Apeza Mayankho, 12/8

CHUMA NDI NTCHITO

Malonda Apadziko Lonse, 9/8

Yuro—Ndalama Yatsopano, 5/8

LINGALIRO LA BAIBULO

Kodi Akufa Ayenera Kulemekezedwa? 2/8

Kodi Chimachititsa Ufiti N’chiyani? 11/8

Kodi Mzimu Woyera wa Mulungu N’chiyani? 1/8

Kodi Nzika Yabwino Imakhala Yotani? 9/8

Kugwirizana pa Zachipembedzo m’Banja, 8/8

Kunyada N’kulakwa? 7/8

Kusankha Wokwatirana Naye, 10/8

Mafumu Atatu Anakaona Yesu ku Betelehemu? 12/8

Misa (Yachikatolika), 5/8

Ndinu Wofunika Kwambiri kwa Mulungu! 6/8

N’kulakwa Kutchula Dzina la Mulungu? 3/8

MAUNANSI A ANTHU

Agogo, 4/8

Asonyezeni Kuti Mumawakonda (achikulire), 4/8

Kalata kwa Makolo Awo (Spain), 3/8

Kusankha Wokwatirana Naye, 10/8

Pamene Mwamuna Kapena Mkazi Akhala Wosakhulupirika, 5/8

MAYIKO NDI ANTHU

India ndi China Akuwonongedwa ndi Fodya, 11/8

Malo Otchuka Achikale Otchedwa Vinland, 7/8

Ndalama ya mu Afirika (peni ya Kissi), 4/8

Njira ya ku Afirika Yopangira Chiponde, 9/8

Phiri la Sinai—Mwala Wokongoletsa Chipululu, 5/8

MBONI ZA YEHOVA

Akazi Anachita Mbali Yaikulu (Zimbabwe), 7/8

Analimbikitsidwa ndi Chikhulupiriro cha Iye, 11/8

“Chikhumbo Changa Chachikulu,” 10/8

Galamukani! Ithandiza Kujambula Chikwangwani Choletsa Kusuta Fodya, 7/8

‘Imapindulitsa Bwanji Anthu?’ 6/8

Kalata kwa Makolo Awo (Spain), 3/8

Mbewu Zimene Zinabala Zipatso Patapita Zaka Zambiri, 7/8

Msonkhano wa za Opaleshoni Yopanda Magazi (Moscow), 5/8

Mulungu Wakhala Mthandizi Wathu (Mozambique), 7/8

NKHANI ZA MOYO WA ANTHU

Anatitengera ku Ukapolo ku Siberia! (V. Kalin), 5/8

Kulera Ana Asanu ndi Aŵiri (B. ndi M. Dickman), 1/8

Kulera Ana mu Afirika (C. McLuckie), 12/8

Kutumikira Mulungu Poyang’anizana ndi Imfa (J. Mancoca), 9/8

Mkango Wobangula Usanduka Mwana wa Nkhosa Wofatsa (E. Torres), 8/8

Mulungu Wakhala Mthandizi Wathu (F. Coana), 7/8

Ndikuthokoza Yehova Kaamba ka Ana Anga Aamuna Asanu (H. Saulsbery), 4/8

Ngakhale Ndili Wakhungu Ndili Wofunika ndi Wachimwemwe (P. Venetsianos), 2/8

UMOYO NDI MANKHWALA

Ana ndi Ngozi, 10/8

Chithandizo Chopanda Magazi, 3/8

Chiyembekezo kwa Opunduka (kuduka chiŵalo), 6/8

Kodi Kuika Anthu Magazi N’kofunikadi? 9/8

Kodi Moyo Wanu Ukukuvulazani? 7/8

Magazi Amatenda, 7/8

Makemikolo, 1/8

Malo Okuzungulirani—Mmene Amakhudzira Thanzi Lanu, 7/8

Moyo Wautali Komanso Wabwino, 8/8

Msonkhano wa za Opaleshoni Yopanda Magazi (Moscow), 5/8

“Mwana Wanu Ali ndi Matenda a Shuga!” 10/8

Njira Yolimbana ndi TB, 6/8

Okonda Kuothera Dzuŵa—Tetezani Khungu Lanu! 7/8

Vuto la Kadyedwe, 2/8

ZINYAMA NDI ZOMERA

Mankhwala Ophera Tizilombo, 3/8

Mtedza Wotchedwa Tagua, 11/8

Wamkulu Kwambiri, Wamng’ono Kwambiri (agulugufe), 9/8

ZOCHITIKA ZA DZIKO NDI MIKHALIDWE YAKE

Ana Ali Pavuto, 4/8

Kuopa Nyukiliya, 9/8

Mankhwala Osokoneza Bongo, 11/8

Nkhondo Idzathadi? 10/8

Ukapolo wa Ana, 6/8

Zaka za Zana la 20—Zaka za Kusintha Kwakukulu, 12/8

ZOSIYANASIYANA

Angelo, 12/8

Chinthu Chamtengo Wapatali Kuposa Ndalama, 10/8

Chofalitsa Chokhala ndi Cholinga, 8/8

Kuuluka, 3/8

Linapulumutsa Ndalama za Munthu Wina, 4/8

“Muli Chidziŵitso Chabwino Bwanji!” 9/8

Nyimbo, 10/8

Zikhulupiriro, 11/8

Zovala Zimene Timavala, 2/8

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena