Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • tr tsamba 191
  • “Pitirizani Kutsata Ukulu Msinkhu”!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Pitirizani Kutsata Ukulu Msinkhu”!
  • Coonadi Cimene Cimatsogolera ku Moyo Wamuyaya
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • “Zinthu Ziwiri Zosasinthika, M’mene Mulungu Sakhoza Kunama”
  • Mtendere Weniweni ndi Chisungiko Zayandikira!
    Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?
  • Kuyang’ana Kuposa pa “Mtendere ndi Chisungiko” Zaumunthu
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Chidziwitso cha pa nthawi yake kaamba ka Ang’ono ndi Akulu
    Mbiri Yabwino Yokusangalatsani
Coonadi Cimene Cimatsogolera ku Moyo Wamuyaya
tr tsamba 191

“Pitirizani Kutsata Ukulu Msinkhu”!

Tsopano popeza kuti mwaziphunzira zoonadi zina zamaziko za Baibulo, inu mufunikira kupitirizabe mu’kukula kwauzimu. Cotero inuyo mudzafuna kucita monga momwe mtumwi Paulo analangizira: “Mwa ici, polekana nao mau a ciyambidwe ca Kristu, tipitirire kutsata ukulu msinkhu.”—Ahebri 6:1.

Kukuthandizani inu kuti mutero, ife tikukulimbikitsani kuti muwerenge bukhu lopatsa cidziwitso ili:

“Zinthu Ziwiri Zosasinthika, M’mene Mulungu Sakhoza Kunama”

Cothandizira phunziro la Baibulo cofunika ici cidzakuthangatani inu kuufikira ukulu msinkhu, popeza kuti pakati pa zinthu zina, cimakupatsani inu: Cidziwitso copita patsogolo ndi kuwazindikira mokulira Mau a Mulungu a coonadi. Cithunzi cabwino kwambiri ca Baibulo lonse lathunthu. Mayankho ocokera ku Magwero apamwambamwamba a zothetsa nzeru zotayitsa mtima za masiku anozi. Liri ndi cikuto colimba ndi masamba 412. Liri ndi zithunzi zokongola. Tumizani 40c (Zambia 40n) tsopano kaamba ka kope lanu, simudzalipira ndarama zopositira.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena