Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • jy tsamba 2-5
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
  • Timitu
  • GAWO 1​—ZIMENE ZINACHITIKA YESU ASANAYAMBE UTUMIKI WAKE
  • GAWO 2​—MMENE UTUMIKI WA YESU UNAYAMBIRA
  • GAWO 3​—YESU ANALALIKIRA KWAMBIRI KU GALILEYA
  • GAWO 4​—YESU ANAKALALIKIRA KU YUDEYA CHAKUMAPETO KWA UTUMIKI WAKE
  • GAWO 5​—YESU ANAKALALIKIRA KUM’MAWA KWA YORODANO CHAKUMAPETO KWA UTUMIKI WAKE
  • GAWO 6​—ZIMENE YESU ANACHITA KUMAPETO KWA UTUMIKI WAKE
Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
jy tsamba 2-5

Zamkatimu

TSAMBA MUTU

GAWO 1​—ZIMENE ZINACHITIKA YESU ASANAYAMBE UTUMIKI WAKE

10 1 Mauthenga Awiri Ochokera kwa Mulungu

12 2 Yesu Analemekezedwa Asanabadwe

14 3 Kubadwa kwa Wokonza Njira

16 4 Mariya Anakhala ndi Pakati Asanakwatiwe

18 5 Kodi Yesu Anabadwa Liti Ndipo Anabadwira Kuti?

20 6 Mwana Amene Mulungu Analonjeza

22 7 Okhulupirira Nyenyezi Anapita Kukaona Yesu

24 8 Anathawa Mfumu Yankhanza

26 9 Yesu Anakulira ku Nazareti

28 10 Yosefe ndi Banja Lake Anapita ku Yerusalemu

30 11 Yohane M’batizi Anakonza Njira

GAWO 2​—MMENE UTUMIKI WA YESU UNAYAMBIRA

34 12 Zimene Zinachitika Pamene Yesu Ankabatizidwa

36 13 Zimene Yesu Anachita Atayesedwa

38 14 Yesu Anayamba Kupeza Ophunzira

40 15 Chozizwitsa Choyamba Chimene Yesu Anachita

42 16 Yesu Anali Wodzipereka pa Kulambira Mulungu

44 17 Yesu Anaphunzitsa Nikodemo Usiku

46 18 Ntchito ya Yesu Inayamba Kuwonjezeka Kuposa ya Yohane

48 19 Yesu Analalikira Mayi wa ku Samariya

GAWO 3​—YESU ANALALIKIRA KWAMBIRI KU GALILEYA

54 20 Chozizwitsa Chachiwiri Chimene Yesu Anachita ku Kana

56 21 Zimene Zinachitika Yesu Ali ku Sunagoge wa ku Nazareti

58 22 Ophunzira 4 Anakhala Asodzi a Anthu

60 23 Yesu Anachita Zozizwitsa Ali ku Kaperenao

62 24 Yesu Analalikira M’madera Ambiri a ku Galileya

64 25 Yesu Anachitira Chifundo Munthu Wakhate N’kumuchiritsa

66 26 “Machimo Ako Akhululukidwa”

68 27 Yesu Anaitana Mateyu

70 28 N’chifukwa Chiyani Ophunzira a Yesu Sankasala Kudya?

72 29 Kodi Kunali Kulakwa Kugwira Ntchito Yabwino pa Tsiku la Sabata?

74 30 Kodi Pali Ubale Wotani Pakati pa Yesu ndi Mulungu?

76 31 Anabudula Ngala za Tirigu pa Tsiku la Sabata

78 32 Kodi Malamulo Ankalola Munthu Kuchita Chiyani pa Tsiku la Sabata?

80 33 Ulosi wa Yesaya Unakwaniritsidwa

82 34 Yesu Anasankha Atumwi 12

84 35 Ulaliki Wotchuka wa Paphiri

92 36 Kapitawo wa Asilikali Anasonyeza Kuti Anali ndi Chikhulupiriro

94 37 Yesu Anaukitsa Mwana Wamwamuna wa Mzimayi Wamasiye

96 38 Yohane Ankafuna Kumva Kuchokera kwa Yesu

98 39 Tsoka kwa M’badwo Umene Sunamvere

100 40 Anawaphunzitsa Kukhululukira Ena

102 41 Kodi Yesu Ankazitenga Kuti Mphamvu Zochitira Zozizwitsa?

104 42 Yesu Anadzudzula Afarisi

106 43 Mafanizo Ofotokoza za Ufumu

112 44 Yesu Analetsa Mphepo Yamphamvu Panyanja

114 45 Anatulutsa Ziwanda Zambiri

116 46 Anachira Atagwira Malaya a Yesu

118 47 Kamtsikana Kanakhalanso ndi Moyo

120 48 Yesu Anachita Zozizwitsa Koma Anakanidwa Ngakhale Kwawo ku Nazareti

122 49 Analalikira ku Galileya Komanso Anaphunzitsa Atumwi

124 50 Anawakonzekeretsa Kuti Azilalikira Ngakhale Pamene Akuzunzidwa

126 51 Anaphedwa pa Tsiku Lokondwerera Kubadwa

128 52 Anadyetsa Anthu Masauzande Ambiri ndi Mikate Komanso Nsomba Zochepa

130 53 Wolamulira Amene Akhoza Kulamulira Mphepo Yamphamvu

132 54 Yesu Ndiye “Chakudya Chopatsa Moyo”

134 55 Anthu Ambiri Anakhumudwa ndi Zimene Yesu Ananena

136 56 Kodi Chimaipitsa Munthu N’chiyani?

138 57 Yesu Anachiritsa Mtsikana Komanso Munthu Wogontha

140 58 Anachulukitsa Mikate Komanso Anachenjeza Ophunzira Ake za Zofufumitsa

142 59 Kodi Mwana wa Munthu Ndi Ndani?

144 60 Anaona Ulemelero wa Khristu Atasandulika

146 61 Yesu Anachiritsa Mnyamata Amene Anali ndi Chiwanda

148 62 Kufunika Kokhala Wodzichepetsa

150 63 Zoyenera Kuchita Anthu Akakhumudwitsana Komanso Wina Akachita Tchimo

152 64 Kufunika Kokhululukira Ena

154 65 Yesu Anaphunzitsa Anthu Ena Ali pa Ulendo Wopita ku Yerusalemu

GAWO 4​—YESU ANAKALALIKIRA KU YUDEYA CHAKUMAPETO KWA UTUMIKI WAKE

158 66 Zimene Zinachitika Yesu Atapita ku Chikondwerero cha Misasa ku Yerusalemu

160 67 “Palibe Munthu Amene Analankhulapo Ngati Iyeyo”

162 68 Mwana wa Mulungu Ndiye “Kuwala kwa Dziko”

164 69 Kodi Atate Wawo Anali Abulahamu Kapena Mdyerekezi?

166 70 Yesu Anachiritsa Munthu Amene Anabadwa Wosaona

168 71 Afarisi Anatsutsana ndi Munthu Amene Anali Wakhungu

170 72 Yesu Anatumiza Ophunzira 70 Kuti Akalalikire

172 73 Nkhani ya Msamariya Imatithandiza Kudziwa Mnzathu Weniweni

174 74 Zimene Tikuphunzira pa Nkhani Yochereza Alendo Komanso ya Pemphero

176 75 Yesu Ananena Zimene Zimachititsa Munthu Kukhala Wodala

178 76 Anakadya Kunyumba kwa Mfarisi

180 77 Yesu Anapereka Malangizo pa Nkhani ya Chuma

182 78 Woyang’anira Nyumba Wokhulupirika Ayenera Kukhala Wokonzeka

184 79 Ayuda Ankayembekezera Kuwonongedwa

186 80 M’busa Wabwino Komanso Makola Awiri a Nkhosa

188 81 Yesu Si Mulungu Koma Iye ndi Atate Wake Ndi Amodzi

GAWO 5​—YESU ANAKALALIKIRA KUM’MAWA KWA YORODANO CHAKUMAPETO KWA UTUMIKI WAKE

192 82 Zimene Zinachitika Pamene Yesu Ankalalikira ku Pereya

194 83 Kuitanira Anthu ku Chakudya

196 84 Kukhala Wophunzira wa Yesu ndi Udindo Waukulu

198 85 Pamakhala Chisangalalo Munthu Wochimwa Akalapa

200 86 Mwana Wotayika Anabwerera

204 87 Muzichita Zinthu Mwanzeru Pokonzekera Zakutsogolo

206 88 Mmene Zinthu Zinasinthira kwa Munthu Wachuma Komanso kwa Lazaro

210 89 Anaphunzitsa ku Pereya Ali pa Ulendo Wopita ku Yudeya

212 90 Yesu Ndi “Kuuka ndi Moyo”

214 91 Yesu Anaukitsa Lazaro

216 92 Pa Anthu 10 Akhate, Mmodzi Anathokoza Yesu

218 93 Mwana wa Munthu Adzaonekera

220 94 Kupemphera Komanso Kudzichepetsa ndi Zinthu Ziwiri Zofunika Kwambiri

222 95 Anawafotokozera Chifukwa Chothetsera Banja Komanso Kuti Azikonda Ana

224 96 Yesu Anayankha Wolamulira Wachinyamata Amene Anali Wolemera

226 97 Fanizo la Anthu Ogwira Ntchito M’munda wa Mpesa

228 98 Atumwi Anasonyezanso Kuti Ankafuna Udindo Wapamwamba

230 99 Yesu Anachiritsa Anthu Akhungu Komanso Anathandiza Zakeyu

232 100 Fanizo la Ndalama 10 za Mina

GAWO 6​—ZIMENE YESU ANACHITA KUMAPETO KWA UTUMIKI WAKE

236 101 Yesu Anakadya Chakudya ku Nyumba kwa Simoni ku Betaniya

238 102 Mfumu Inalowa mu Yerusalemu Itakwera pa Bulu

240 103 Yesu Anayeretsanso Kachisi

242 104 Kodi Ayuda Anakhulupirira Yesu Atamva Mulungu Akulankhula?

244 105 Yesu Anagwiritsa Ntchito Mtengo wa Mkuyu Pophunzitsa Anthu za Chikhulupiriro

246 106 Mafanizo Awiri Onena za Munda wa Mpesa

248 107 Mfumu Inaitanira Anthu ku Phwando la Ukwati

250 108 Yesu Analepheretsa Afarisi Kuti Amugwire

252 109 Anadzudzula Atsogoleri Achipembedzo Omwe Ankamutsutsa

254 110 Tsiku Lomaliza Limene Yesu Anapezeka pa Kachisi

256 111 Atumwi Anapempha Chizindikiro

260 112 Fanizo la Anamwali Limatiphunzitsa Kufunika Kokhala Tcheru

262 113 Fanizo la Matalente Limatiphunzitsa Kufunika Kochita Zinthu Mwakhama

264 114 Khristu Akadzayamba Kulamulira Adzaweruza Nkhosa ndi Mbuzi

266 115 Yesu Anachita Mwambo Womaliza wa Pasika

268 116 Anawaphunzitsa Kudzichepetsa pa Pasika Womaliza

270 117 Chakudya Chamadzulo cha Ambuye

272 118 Anakangananso Kuti Wamkulu Ndani

274 119 Yesu​—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo

276 120 Anali Ngati Nthambi Zobala Zipatso Komanso Anali Mabwenzi a Yesu

278 121 “Limbani Mtima Ndaligonjetsa Dziko”

280 122 Pemphero Lomaliza la Yesu Ali M’chipinda Chapamwamba

282 123 Anapemphera Pamene Anali ndi Chisoni Kwambiri

284 124 Khristu Anaperekedwa Kenako Anamangidwa

286 125 Atamugwira Anapita Naye kwa Anasi Kenako kwa Kayafa

288 126 Petulo Anakana Yesu Kunyumba kwa Kayafa

290 127 Khoti la Sanihedirini Linaweruza Mlandu wa Yesu Kenako Anapita Naye kwa Pilato

292 128 Pilato Komanso Herode Sanamupeze Yesu ndi Mlandu

294 129 Pilato Ananena Kuti: “Taonani! Mwamuna Uja Ndi Uyu!”

296 130 Pilato Anapereka Yesu Ndipo Anthu Anamutenga Kuti Akamuphe

298 131 Mfumu Yosalakwa Inavutika Itapachikidwa Pamtengo

300 132 “Ndithudi Munthu Uyu Analidi Mwana wa Mulungu”

302 133 Anakonza Thupi la Yesu ndi Kukaliika M’manda

304 134 M’manda a Yesu Munalibe Kanthu Chifukwa Anali Ataukitsidwa

306 135 Yesu Ataukitsidwa Anaonekera kwa Anthu Ambiri

308 136 Anaonekera M’mbali Mwanyanja ya Galileya

310 137 Anaonekera kwa Anthu Ambiri Mwambo wa Pentekosite Usanachitike

312 138 Khristu Anakhala Kudzanja la Manja la Mulungu

314 139 Yesu Adzabweretsa Paradaiso Kenako Adzamaliza Kugwira Ntchito Imene Anapatsidwa

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena