Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CA-copgm17 tsamba 4
  • Muzimvetsera Mwachidwi Kuti Mupeze Mayankho a Mafunso Awa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzimvetsera Mwachidwi Kuti Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wadera ya 2016-2017—Wokhala ndi Woyang’anira Dera
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Thamangani N’cholinga Choti Mukalandire Mphoto’
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Muzikhala ndi Makhalidwe Amene Mulungu Amasangalala Nawo​—Chikhulupiriro
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Kodi Mumakhulupiriradi Uthenga Wabwino?
    Nsanja ya Olonda—2003
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wadera ya 2016-2017—Wokhala ndi Woyang’anira Dera
CA-copgm17 tsamba 4

Muzimvetsera Mwachidwi Kuti Mupeze Mayankho a Mafunso Awa:

  1. N’chifukwa chiyani tiyenera kukhulupirira Mulungu nthawi zonse? (Maliko 11:22)

  2. Kodi kuganizira mawu oyerekezera ofotokoza za Yehova kungatithandize bwanji? (Sal. 28:7; Luka 11:11-13; Deut. 32:4; Sal. 23:1)

  3. Kodi tingalimbitse bwanji chikhulupiriro chathu? (Maliko 9:24)

  4. Kodi “tchimo limene limatikola mosavuta” ndi liti, ndipo tingalipewe bwanji? (Aheb. 12:1)

  5. N’chiyani chikutitsimikizira kuti anthu amene ali ndi chikhulupiriro cholimba adzalandira mphoto? (Aheb. 11:6)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena