Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm19 tsamba 2-3
  • Lachisanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lachisanu
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • MASANA
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2022
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2017
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
CO-pgm19 tsamba 2-3

Lachisanu

‘MULUNGU AMATIPHUNZITSA KUKONDANA’​—1 ATESALONIKA 4:9

M’MAWA

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 105 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YA TCHEYAMANI: N’chifukwa Chiyani “Chikondi Sichitha”? (Aroma 8:38, 39; 1 Akorinto 13:1-3, 8, 13)

  • 10:15 NKHANI YOSIYIRANA: Samalani Kuti Musamadalire Zinthu Zimene Zimatha

    • Chuma (Mateyu 6:24)

    • Udindo Komanso Kutchuka (Mlaliki 2:16; Aroma 12:16)

    • Nzeru za Anthu (Aroma 12:1, 2)

    • Mphamvu Komanso Kukongola (Miyambo 31:30; 1 Petulo 3:3, 4)

  • 11:05 Nyimbo Na. 40 ndi Zilengezo

  • 11:15 KUWERENGA BAIBULO MWASEWERO: Yehova Anapitiriza Kusonyeza Chikondi Chokhulupirika (Genesis 37:1-36; 39:1–47:12)

  • 11:45 Yehova Amakonda Anthu Amene Amakonda Mwana Wake (Mateyu 25:40; Yohane 14:21; 16:27)

  • 12:15 Nyimbo Na. 20 ndi Kupuma

MASANA

  • 1:25 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:35 Nyimbo Na. 107

  • 1:40 NKHANI YOSIYIRANA: Chikondi Chanu Chisathe Ngakhale Kuti . . .

    • Munakulira M’banja Lopanda Chikondi (Salimo 27:10)

    • Mukukumana ndi Mavuto Kuntchito (1 Petulo 2:18-20)

    • Mukukumana ndi Mavuto Kusukulu (1 Timoteyo 4:12)

    • Mukudwala Matenda Okhalitsa (2 Akorinto 12:9, 10)

    • Mukuvutika ndi Umphawi (Afilipi 4:12, 13)

    • Mukutsutsidwa ndi a M’banja Lanu (Mateyu 5:44)

  • 2:50 Nyimbo Na. 141 ndi Zilengezo

  • 3:00 NKHANI YOSIYIRANA: Chilengedwe Chimasonyeza Kuti Yehova Ndi Wachikondi

    • Kumwamba (Salimo 8:3, 4; 33:6)

    • Dziko Lapansi (Salimo 37:29; 115:16)

    • Zomera (Genesis 1:11, 29; 2:9, 15; Machitidwe 14:16, 17)

    • Zinyama (Genesis 1:27; Mateyu 6:26)

    • Thupi la Munthu (Salimo 139:14; Mlaliki 3:11)

  • 3:55 “Yehova Amalanga Aliyense Amene Iye Amamukonda” (Aheberi 12:5-11; Salimo 19:7, 8, 11)

  • 4:15 “Valani Chikondi” (Akolose 3:12-14)

  • 4:50 Nyimbo Na. 130 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena