Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm22 tsamba 4-5
  • Loweruka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Loweruka
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2022
  • Nkhani Yofanana
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2022
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2022
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2022
CO-pgm22 tsamba 4-5
Malo a mtundu wa buluu komanso wa girini.

Loweruka

“Adzakupezeni opanda banga, opanda chilema ndiponso muli mu mtendere”​—2 Petulo 3:14

M’Mawa

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 58 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YOSIYIRANA: Muzikhala Okonzeka Kulalikira “Uthenga Wabwino Wamtendere”

    • • Pitirizani Kuchita Khama (Aroma 1:14, 15)

    • • Muzikonzekera Mokwanira (2 Timoteyo 2:15)

    • • Muziyamba Ndinu Kuwalankhula (Yohane 4:6, 7, 9, 25, 26)

    • • Muzibwereranso Kwa Anthu Achidwi (1 Akorinto 3:6)

    • • Muzithandiza Ophunzira Anu Kuti Akhale Olimba (Aheberi 6:1)

  • 10:40 Achinyamata​—Sankhani Njira Yomwe Ingakubweretsereni Mtendere (Mateyu 6:33; Luka 7:35; Yakobo 1:4)

  • 11:00 Nyimbo Na. 135 ndi Zilengezo

  • 11:10 VIDIYO: Mmene Abale Athu Akukhalira Mwamtendere Ngakhale Kuti . . .

    • • Akutsutsidwa

    • • Akudwala

    • • Akukumana ndi Mavuto a Zachuma

    • • Akukumana ndi Ngozi Zam’chilengedwe

  • 11:45 NKHANI YA UBATIZO: Pitirizani Kuyenda “Panjira Yamtendere” (Luka 1:79; 2 Akorinto 4:16-18; 13:11)

  • 12:15 Nyimbo Na. 54 ndi Kupuma

Masana

  • 1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:45 Nyimbo Na. 29

  • 1:50 NKHANI YOSIYIRANA: Muzipewa Zinthu Zomwe Zingasokoneze Mtendere

    • • Kudzitama (Aefeso 4:22; 1 Akorinto 4:7)

    • • Nsanje (Afilipi 2:3, 4)

    • • Zachinyengo (Aefeso 4:25)

    • • Miseche (Miyambo 15:28)

    • • Mkwiyo (Yakobo 1:19)

  • 2:45 VIDIYO YA NKHANI YA M’BAIBULO: Yehova Amatitsogolera Panjira Yamtendere—Mbali Yoyamba (Yesaya 48:17, 18)

  • 3:15 Nyimbo Na. 130 ndi Zilengezo

  • 3:25 NKHANI YOSIYIRANA: Muzifunafuna “Mtendere ndi Kuusunga” . . .

    • • Musamakwiye Msanga (Miyambo 19:11; Mlaliki 7:9; 1 Petulo 3:11)

    • • Muzipepesa (Mateyu 5:23, 24; Machitidwe 23:3-5)

    • • Muzikhululuka ndi Mtima Wonse (Akolose 3:13)

    • • Muzigwiritsa Ntchito Mwanzeru Mphatso ya Kulankhula (Miyambo 12:18; 18:21)

  • 4:15 Muziteteza “Umodzi Wathu Pokhala Mwamtendere” (Aefeso 4:1-6)

  • 4:50 Nyimbo Na. 113 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena