Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w90 12/15 tsamba 31
  • Chosonyezera Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1990

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chosonyezera Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1990
  • Nsanja ya Olonda​—1990
  • Timitu
  • BAIBULO
  • CHIDZIŴITSO PA NYUZI
  • LIPOTI LA OLENGEZA UFUMU
  • MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA
  • MALO KUCHOKERA KU DZIKO LOLONJEZEDWA
  • MBIRI YA MOYO WA ANTHU
  • MBONI ZA YEHOVA
  • MOYO NDI UMINISITALA ZA YESU
  • MOYO WACHIKRISTU NDI MIKHALIDWE
  • NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRIDWA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • YEHOVA
  • YESU KRISTU
Nsanja ya Olonda​—1990
w90 12/15 tsamba 31

Chosonyezera Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1990

Chosonyeza deti la kope limene nkhaniyo ikupezeka

BAIBULO

Bukhu Lamakedzana la Bezae, 2/15

Bukhu lamakedzana la Washington, 6/1

Kodi mungalikhulupirire Baibulo? 2/1

Kodi Timafunikiradi Oyambirirawo? 7/15

Yohane (Uthenga Wabwino), 3/15

Machitidwe, 5/15, 6/1, 6/15

Aroma 8/1

1 Akorinto, 9/15

2 Akorinto, 9/15

Agalatiya, 11/15

Aefeso, 11/15

Afilipi, 11/15

Akolose, 11/15

CHIDZIŴITSO PA NYUZI

2/15, 3/15, 5/15, 6/15, 7/15, 9/15, 10/15, 11/15, 12/15

LIPOTI LA OLENGEZA UFUMU

1/1, 3/1, 4/1, 5/1, 6/1, 7/1, 8/1, 9/1, 12/1

MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA

Kodi anthu ambiri oukitsidwa adzakana chowonadi? 3/15

Kodi liwu Lachigiriki lakuti phronema​—ndilo “tanthauzo” kapena “kusamalira”? 12/1

Kodi liwu Lachigiriki lakuti pisteuo​—ndilo “kukhulupirira” kapena “kusonyeza chikhulupiriro”? 12/1

Kodi majekeseni okhala ndi mbali za mwazi ngolandirika? 6/1

Kodi muyenera kupewa kofi, tiyi? 2/15

Kodi ndiliti pamene malipenga asanu ndi aŵiri anayamba? (Chibv 8-11), 4/1

Kodi njoka “njochenjera”? (Gen 3:1), 10/15

Kodi nkupezekeranji pamaliro? 10/15

Kodi odzozedwa adzapulumuka chisautso chachikulu? 8/15

Kodi Yehova analankhula ndi Adamu mwachindunji? 5/1

Kusaka ndi kusodza, 5/15

MALO KUCHOKERA KU DZIKO LOLONJEZEDWA

Chigwa cha Ela​—Kumene Davide Anaphera Chimphona! 1/1

Kodi Mudzaphunzira Kuchokera Kunyengo? 9/1

Kuchokera pa Tabori Kutsikira ku Chilakiko! 5/1

Nazarete​—Kwawo kwa Mneneri, 3/1

Samariya​—Likulu Pakati pa Malikulu Akumpoto, 11/1

Yordano Amene Simungamdziŵe, 7/1

MBIRI YA MOYO WA ANTHU

Kuchita ndi Zofooka Zanga (T. Addison), 5/1

Kukhulupirira Yehova Kumadzetsa Chimwemwe (J. H. Nathan), 9/1

Kusangalala ndi Kututa mu India (F. E. Skinner), 1/1

Kutumikira Katswiri Wojambula Kuposa Onse, 4/1

Kutumikira Yehova m’Nyengo Yabwino ndi m’Nyengo Yovuta (H. Bently), 6/1

Madalitso A Yehova Andilemeretsa (E. Meynberg), 7/1

Ndaiwona Ikukula Kum’mwera kwa Africa (R. A. McLuckie), 2/1

‘Ndinauluka Pamwamba ndi Mapiko Monga Ziwombankhanga’ (I. Berg), 4/1

Tinalera Ana Asanu ndi Atatu M’chilangizo cha Yehova (O. Menezes), 8/1

Yehova Anadalitsa Kutsimikiza Mtima Kwanga (R. Wuttke), 10/1

Yehova Wandipatsa Nyonga (E. Okoka), 12/1

MBONI ZA YEHOVA

Chifukwa Chake Réunion Ili ndi Nyumba Zaufumu Zambiri, 9/15

Chikristu Chowona Chikuwongolera Moyo m’Sweden, 5/15

Chizunzo Chipitirizabe mu Burundi, 1/1

Chochita Chanzeru Tsoka Lisanakanthe, 7/15

Kuchereza kwa Melita Kudzetsa Madalitso, 7/15

“Kuchirimika Monga Gulu Limodzi Lankhosa” mu Chad, 10/15

Kuchitira Umboni M’malo Abizinezi​—Njira Yachijapan, 2/1

Kudzipereka Kwaumulungu​—Kopindulitsa Zinthu Zonse (Poland), 1/15

Kufalitsa kwa Padziko Lonse kwa Mbiri Yabwino, 1/1

Kugwa kwa Babulo kufalitsidwa mu Japan, 3/1

Kugwira Ntchito ya Mulungu M’njira ya Mulungu mu Nigeria, 8/15

Kumaliza Maphunziro a Gileadi, 6/1, 12/15

‘Kusodza Anthu’ mu Belize, 4/15

Kututa Zochuluka Kubweretsa Chisangalalo mu Taiwan, 11/15

Lipoti Lautumiki la Chaka, 1/1

Mmene Yehova Amapititsira Patsogolo Ntchito Yake, 12/1

Sierra Leone​—“Madiamond” Ake Amtengo Koposa, 3/15

“Tsopano Tiri ndi Nyumba Yaufumu Yathu Yathu,” 5/1

MOYO NDI UMINISITALA ZA YESU

(Nkhani zowonekera m’kope lirilonse.)

MOYO WACHIKRISTU NDI MIKHALIDWE

“Chirimikani”​—Musakhumudwe, 4/15

Kodi Mudzapindula ndi Chisomo?, 2/15

Kodi Mumatsatira Malangizo? 10/1

Kodi Nkulondoleranji Chilungamo? 10/15

Kumbukirani Mlengi Wanu Wamkulu Muunyamata Wanu, 5/15

Kusunga Nthaŵi ndi Inu, 6/15

Kuthandiza Ochita Tondovi Kupezanso Chimwemwe, 3/15

Kuwona Mtima Kuli Lamulo Labwino Koposa, 3/1

Lamulirani Mkwiyo Wanu! 9/15

Lemekezani Yehova ndi Chuma Chanu, 7/1

Musanyalanyaze Mnzanu! 8/15

‘Pemphereranani,’ 11/15

Pitirizanibe Kuyenda m’Chowonadi, 9/1

‘Pitirizani Kukhala Wowongolereka,’ 11/1

Tsitsimulani Achibale Anu, 2/15

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRIDWA

Achichepere Achimwemwe mu Utumiki wa Yehova, 8/1

‘Achimwemwe Ali Awo Amene Apirira,’ 1/1

Anthu a Yehova Alimbitsidwa m’Chikhulupiriro, 6/15

‘Chachikulu cha Izi Ndicho Chikondi,’ 11/15

Chikondi Chenicheni Chimafupa, 11/15

Chilungamo Osati Miyambo Yapakamwa, 10/1

Chinsinsi Chopatulika Chivumbuluka, 1/15

Chipulumutso Chiri Pafupi kwa Anthu Odzipereka Mwaumulungu! 4/15

Chiweruzo cha Mulungu Motsutsana Ndi “Munthu Wosayeruzika,” 2/1

Chuma Chathu, Uminisitala Wamakono Waulemerero, 7/15

Dalitsani Dzina Loyera la Yehova! 9/15

Iwo Anachivomereza Chikondi cha Mulungu Mopanda Dyera, 12/1

‘Kapolo Wokhulupirika’ ndi Bungwe Lake Lolamulira, 3/15

Kawonedwe ka Mkristu ka Maulamuliro Aakulu, 11/1

Kawonedwe Kanu ka Moyo kamayambukira Moyo Wanu, 5/1

Khalani Akuchita Mawu, Osati Akumva Okha, 10/1

Khalani Oyamikira​—Ufumu Waumesiya wa Yehova Ukulamulira, 10/15

Kodi Mukukalimira? 9/1

Kodi Muli Woyeneretsedwa Kutumikira? 9/1

Kodi Mumayamikira Zimene Mulungu Wachita? 8/1

Kodi Tingavomereze Motani Chikondi cha Mulungu Mopanda Dyera? 12/1

Konzekerani Kaamba ka Chipulumutso Kuloŵa m’Dziko Latsopano, 4/15

Kuchokera ku Seder Kumka ku Chipulumutso, 2/15

Kugonjera Kwathu Kochepa ku Maulamuliro Aakulu, 11/1

Kugwira Ntchito ndi Yehova Mokhulupirika, 8/15

Kugwirizana ndi Bungwe Lolamulira Lerolino, 3/15

Kukhulupirika​—Pamtengo Wotani? 8/15

Kuphunzira Chinsinsi Chopatulika cha Kudzipereka Kwaumulungu, 1/15

Kuthetseratu Nkhani ya Chilengedwe Chonse, 7/1

Kuvumbula “Munthu Wosayeruzika,” 2/1

Kuwanditsa Fungo Lokoma la Chidziŵitso Chonena za Mulungu, 7/15

Kuyamikira Chifukwa Chimene Mesiya Ankadzera, 10/15

Kuzindikira “Munthu Wosayeruzika,” 2/1

‘Kuzindikira Zimene Ife Tiri’​—Panthawi ya Chikumbutso, 2/15

Lengezani Ufumu wa Yehova Molimba Mtima! 6/15

Limbikitsanani Pamene Tsiku Likuyandikira, 12/15

Londolani Kudzipereka Kwaumulungu Monga Akristu Obatizidwa, 3/1

Mapeto Akudzawo a “Buku la Nkhondo za Yehova,” 7/1

“Mawu a Mulungu Ngamoyo Ndipo Amapereka Mphamvu,” 4/1

Mawu a Mulungu ndi Chowonadi, 4/1

Mawu a Yehova Afalikira! 6/15

Muthange Mwafuna Ufumu ndi chilungamo cha Mulungu, 10/1

Ntchito ya Maulamuliro Aakulu, 11/1

Opani Yehova, Wakumva Pemphero, 5/15

‘Sindichititsidwa Manyazi ndi Mbiri Yabwino,’ 1/1

Sonyezani Chikhulupiriro Kaamba ka Moyo Wosatha, 5/1

“Tiphunzitseni Ife Kupemphera,” 5/15

Tsatirani Chitsanzo cha Yesu cha Kudzipereka Kwaumulungu, 3/1

“Wakumva Anene, Idzani,” 12/15

Yehova Amafunikira Chitamando Chosatha, 9/15

Yehova Ndiye Wolamulira Wathu! 6/1

Yendani M’kuwopa kwa Yehova, 6/1

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Achichepere Omwe Amatumikira Mulungu, 8/1

“Achimwemwe Ngamtendere,” 8/1

Atumiki Achichepere m’Nthaŵi za Baibulo, 8/1

Armagedo​—Liti? 5/15

Betelehemu ndi Krisimasi, 12/15

Chimveni Chowonadi Chonse! 9/15

Chisungiko Chapadziko Lonse​—Motani? 6/15

Chuma Chamtengo Woposa wa Golide! 9/15

Dziko Lopanda Umbombo, 2/15

Kodi Adzatsogolera Anthu ku Mtendere Ndani? 4/1

Kodi Amphaŵi Angathe Kukhala Owona Mtima? 11/15

Kodi Kuikidwiratu Kuyenera Kulamulira Moyo Wanu? 8/15

Kodi Moyo Umapulumuka pa Imfa? 9/1

Kodi ndi Mapemphero Andani Amene Amayankhidwa? 1/15

Kodi Ndi Mulungu Uti Amene Mumamlambira? 12/1

Kodi Ndi Mulungu Uti Amene Muyenera Kulambira? 12/1

Kufunafuna Chisungiko, 6/15

‘Kufunafuna Mawu Okondweretsa, Mawu Owongoka,’ 12/15

Kupambana Nkhondo Yolimbana ndi Kuchita Tondovi, 3/1

Kupeza Chimwemwe​—Koma Kuti? 3/1

Kusintha Chibadwa cha Anthu, 11/1

Kutembenuzidwa kwa Constantine​—Ku Chiyani? 1/15

‘Kutsutsa​—Chotchedwa Chidziŵitso Konama’ (Irenaeus), 7/15

Kuwononga Dziko Lapansi, 7/15

“Ligubo Lachigonjetso,” 11/15

Mamiliyoni Amene Ngakufa Tsopano Adzakhalanso Ndi Moyo, 5/1

Masada, 10/15

Mbiri Yabwino Kaamba ka Mtundu Wonse wa Anthu! 1/1

‛Mitembo Yambiri ya Anthu Oyera Mtima inauka,’ 9/1

‘Mkazi Uja Yezebeli,’ 4/1

Mose Wokhala ndi Nyanga​—Chopeka cha Mmisiri, 3/15

Mtendere​—Kodi Pali Kuthekera Kotani? 4/1

Mtendere wa Dziko Lonse​—Kodi Udzatanthauzanjidi? 4/15

Mungapeze Chimwemwe m’Dziko Lochititsa Tondovi! 3/1

Mwala Wachimoabu, 4/15

Nkhondo ya Yeriko​—Nthano Kapena Yeniyeni? 7/15

Nthaŵi ya Dziko Latsopano, 10/1

“Pambuyo Pake Anapatsanso Mwamuna Wake,” 6/15

‘Phanga la Achifwamba’ Lamakono, 12/15

Posachedwapa​—Dziko Lopanda Zopweteka! 7/15

Tanthauzo la Mwambiwo, 9/15

Umboni wa Ulemerero wa Solomo, 6/15

Yehova Amatidziŵa Bwino! 1/15

Zaka Chikwi Zachitatu​—Kodi Zidzakwaniritsa Ziyembekezo Zanu? 6/1

Zaka Chikwi Zopambana Zikuyandikira, 6/1

YEHOVA

Kodi Nchifukwa Ninji Yehova Wavumbula Dzina Lake? 2/15

YESU KRISTU

Kodi Imfa ya Yesu Imatanthauzanji kwa Inu? 3/15

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena