Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w95 12/15 tsamba 31
  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1995

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1995
  • Nsanja ya Olonda—1995
  • Timitu
  • BAIBULO
  • MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA
  • MBONI ZA YEHOVA
  • MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU
  • NKHANI ZA MOYO WA ANTHU
  • NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRIDWA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA
  • YEHOVA
  • YESU KRISTU
Nsanja ya Olonda—1995
w95 12/15 tsamba 31

Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1995

Zosonyeza deti la kope lopezekamo nkhaniyo

BAIBULO

“Chipangano Chakale” Kapena “Malemba Achihebri”? 3/1

Katswiri Achita Chidwi ndi New World Translation, 4/15

Kodi Baibulo Lili ndi Mtengo Wanji? 3/15

Kodi Malemba a Amasoreti Nchiyani? 5/15

Pamene Amaliŵerenga ndi Mmene Amapindulira 5/1

MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA

‘Asakhale aphunzitsi ambiri’ (Yak. 3:1), 9/15

“Dzina limene liposa maina onse” (Afil. 2:9), 11/15

Kodi Afilisti anali ayani? 2/1

Kodi Mulungu anachita tsankhu posankha bungwe lolamulira loyambirira la Ayuda okhaokha? 7/1

Kodi Mariya anali ndi pakati pamene anachezera Elisabeti? 7/15

Kodi Yesu tsopano ndi mkulu wa ansembe kwa “nkhosa zina”? 6/1

“Mbadwo” (1 Pet. 2:9; Mat. 24:34), 11/1

Mkhalidwe wosonyezedwa pa ubatizo, 4/1

“Mulibe mantha m’chikondi” (1 Yoh. 4:18), “opani Mulungu” (1 Pet. 2:17), 8/1

“Mzimu” wa mu Agalatiya 6:8, 6/15

“Nkhosa zina” ndi “khamu lalikulu” pali kusiyana kodi? 4/15

MBONI ZA YEHOVA

Anazichita Kaamba ka Chikondi (nyumba ya mkazi wamasiye ikonzedwa), 10/15

Atene, Greece, 10/15

Brazil, 7/15

Dominican Republic, 2/15

‘Ha, Bwenzi Aliyense Akanakhala Ngati Iwo!’ 9/1

Ife Sitidzapuma pa Ntchito Yathu! (Japan), 3/15

India, 9/15

“Kodi Ndalamazo Zimachokera Kuti?” 12/1

“Kugulitsa Mchere” m’Mozambique, 4/15

Kukwera Phiri Lalitali Kuposa Mapiri a Himalaya (Nepal), 6/15

Kumaliza Maphunziro a Gileadi, 6/1, 12/1

Misonkhano Yachigawo ya “Mantha Aumulungu,” 1/15

“Mkamwa mwa Makanda,” 1/1

Mlandu wa Mboni za Yehova Ugamulidwa (Greece), 12/15

“Ndine Wamtengo Wapatali Pamaso pa Yehova!” 12/15

New Zealand, 11/15

Nyumba ya Ufumu ku Niue, 12/15

Puerto Rico, 1/15

Singapore Apondereza Ufulu wa Kulambira, 10/1

Sri Lanka, 8/15

Sweden, 5/15

Zambia, 3/15

MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU

Chenjerani ndi Kudzilungamitsa! 10/15

Chilungamo Chimakuza Mtundu, 12/15

Chitonthozo cha Awo a “Mtima Wosweka,” 11/1

Kanizani Miyambo Yachikunja! 8/15

Kodi Mungachititse Motani Mapemphero Anu Kukhala Atanthauzo? 3/15

Kodi Mungakulitse Luntha Lowonjezereka? 9/1

Kodi Mungazime Nyali Yofuka? 11/15

Kodi Mwalimbikitsapo Aliyense Posachedwapa? 1/15

Kodi ndi Mlandu wa Yani? 2/1

Kuchotsa​—Makonzedwe Achikondi? 7/15

Kuleza Mtima​—Nchifukwa Ninji Sikumaonekaoneka? 6/15

Kumvera Kwaumulungu m’Banja la Zipembedzo Zosiyana, 6/1

Kuzindikira Kufooka, Kuipa, ndi Kulapa, 1/1

Mabanja Opembedza Akale, 9/15

Mfupo za Kulimbikira, 8/1

Mmene Akristu Amachitira ndi Chitonzo Chofalitsidwa, 4/1

Mukhoza Kugonjetsa Zopinga Zimenezi! 7/15

‘Musakhale Omangidwa m’Goli Losiyana,’ 11/15

Mzimu Wopatsa, 12/15

Phunziro pa Kusamalira Mavuto, 2/15

Samalirani Changu Chanu, 10/1

Sungani Umphumphu ndi Kukhala ndi Moyo! 1/1

Umbeta m’Nthaŵi za Mavuto a Zachuma, 6/15

NKHANI ZA MOYO WA ANTHU

“Chikondi Sichilephera” (S. Ladesuyi), 9/1

Chinthu Chabwino Koposa Chochita ndi Moyo Wanga (B. Anderson), 3/1

Choloŵa Chathu Chauzimu Chaulemerero (F. Smith), 8/1

Chosankha Changa cha Kufikira Ukulu Msinkhu (C. Dochow), 4/1

Chuma Chosayerekezereka Chogaŵana ndi Ena (G. Malaspina), 1/1

Khama Lichititsa Kupita Patsogolo (J. Maglovsky), 5/1

Kutsatira Mapazi a Makolo Anga (H. Padgett), 10/1

“Popeza Tili Nawo Utumiki. . . . , Sitifooka” (R. Taylor), 2/1

Tinapatsidwa Ngale ya Mtengo Wapatali (R. Gunther), 6/1

Wa Zaka Zana Koma Wolimbabe (R. Mitchell), 12/1

‘Wogwetsedwa, Koma Wosawonongeka’ (U. Helgesson), 11/1

Wokhala Ndekha Koma Wosasiyidwa (A. Lewis), 7/1

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRIDWA

Akazi Achikristu Ayenera Kuchitiridwa Ulemu, 7/15

“Akuchita Mawu” Achimwemwe, 12/15

Chiitano Chachikondi kwa Otopa, 8/15

Chikondi Chimagonjetsa Nsanje Yoipa, 9/15

Chimwemwe cha Yehova Ndicho Linga Lathu, 1/15

Chitonthozo Chochokera kwa “Mulungu wa Chitonthozo Chonse,” 6/1

Fulumizanani ku Chikondano ndi Ntchito Zabwino​—Motani? 4/1

“Goli Langa Lili Lofeŵa, ndi Katundu Wanga Ali Wopepuka,” 8/15

“Israyeli wa Mulungu” ndi “Khamu Lalikulu,” 7/1

Khalani ‘m’Mudzi Wopulumukirako’ Nimukhale ndi Moyo! 11/15

Khamu Lalikulu la Olambira Oona​—Lachokera Kuti? 2/1

Khamu Lalikulu Lopereka Utumiki Wopatulika, 2/1

Kodi Mudzaima Motani ku Mpando wa Chiweruzo? 10/15

Kodi Mulungu Ali Pamalo Oyamba m’Banja Lanu? 10/1

Kodi Nchiyani Chimakusonkhezerani Kutumikira Mulungu? 6/15

Kodi Nkhosazo ndi Mbuzizo Zili ndi Mtsogolo Motani? 10/15

Kuchita Mogwirizana ndi Kudzipatulira Kwathu “Tsiku ndi Tsiku,” 3/1

Kudzakhala Kuuka kwa Olungama, 2/15

Kumlaka Satana ndi Ntchito Zake, 1/1

Kuphunzira Kupeza Chisangalalo m’Kuwopa Yehova, 3/15

Kuphunzitsidwa ndi Yehova Mpaka Lero, 8/1

Kupindula ndi Kuŵerenga Baibulo Tsiku ndi Tsiku, 5/1

Kupulumutsidwa Amoyo Kupyola Chisautso Chachikulu, 2/15

Kuŵala kwa Kuunika​—Kwakukulu ndi Kwakung’ongo (Mbali 1 ndi 2), 5/15

Kuŵala kwa Kuunika m’Nthaŵi za Atumwi, 5/15

Landirani Baibulo Monga Momwe Lililidi, 5/1

Makolo ndi Ana: Ikani Mulungu Pamalo Oyamba! 10/1

Malo Olemekezeka a Akazi Pakati pa Atumiki a Mulungu Oyambirira, 7/15

Mapindu a Kuwopa Mulungu Woona, 3/15

Mboni Zachikristu Zochirikiza Ulamuliro wa Mulungu, 9/1

Mboni Zachikristu Zokhala ndi Unzika Wakumwamba, 7/1

Mboni Zotsutsa Milungu Yonama, 9/1

Midzi Yopulumukirako​—Makonzedwe Achifundo a Mulungu, 11/15

“Momwemo Anachita,” 12/15

Musaleme! 12/1

“Musawopa, Kagulu ka Nkhosa Inu,” 2/15

Mtundu Wosunga Umphumphu, 1/1

Nchifukwa Ninji Tiyenera Kuwopa Mulungu Woona Tsopano? 10/15

Ndinu Wamtengo Wapatali Pamaso pa Mulungu! 4/1

Ngakhale Tilira, Sitili Opanda Chiyembekezo, 6/1

Nsanje ya pa Kulambira Yehova Koyera, 9/15

Nthaŵi ya Kudikira, 11/1

Odzipatulira​—Kwa Yani? 3/1

Okhalira Pamodzi mu “Dziko” Lobwezeretsedwa, 7/1

Opulumuka ku “Mbadwo Woipa,” 11/1

Tsiku Lochititsa Mantha la Yehova Lili Pafupi, 4/15

Tsiku “Lotentha Ngati Ng’anjo,” 4/15

Tumikirani Yehova ndi Chimwemwe cha Mtima, 1/15

“Utumiki Wopatulika ndi Mphamvu Yanu ya Kulingalira,” 6/15

Yehova Amapereka Mphamvu kwa Wotopa, 12/1

Yehova​—Mulungu Amene Amaphunzitsa, 8/1

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Aamoni Anabwezera Udani pa Kukoma Mtima, 12/15

Akaraite ndi Kufunafuna Kwawo Choonadi, 7/15

Akathari​—Kodi Anali Akristu Ofera Chikhulupiriro? 9/1

Akazi Padziko Lonse, 6/15

Amasoreti, 9/15

Analandira Chitsogozo cha Mulungu (Yosefe, Atate Wolera wa Yesu), 1/15

Anali Kalambula Bwalo wa Mesiya (Yohane Mbatizi), 5/15

Angelo, 11/1

Chipembedzo Chanu​—Chombo Chosayenera Kutulukamo? 2/1

Chipembedzo​—Kodi ndi Nkhani Yosayenera Kukambitsirana? 4/1

“Choonadi Nchiyani?” 7/1

Chothetsa Nzeru cha Maphunziro a Zaumulungu (Moyo Wosafa), 3/1

Chotupitsa Mkate cha Afarisi ndi Asaduki, 3/15

Dziko Lopanda Kusaona Mtima, 6/1

Dziko Lopanda Nkhondo​—Lidzafika Liti? 10/1

Kodi Bizinesi Yanu Idzakutayitsani Chiyani? 5/1

Kodi Choonadi cha Chipembedzo Chingapezeke? 4/15

Kodi Mantha Adzatha Liti? 8/15

Kodi Moyo Ngwamtengo Wapatali Motani kwa Inu? 1/15

Kodi Mudzatamanda Yehova? 3/15

Kodi Mulungu Amalamulira Dziko? 7/15

Kodi Mulungu Anaikiratu za Mtsogolo Mwathu? 2/15

Kodi Udani Udzatha Konse? 6/15

Kuikiratu za Mtsogolo, 2/15

Kuthira Mwazi Kupendedwanso, 8/1

Kuunika Kwawo Sikunazime, 11/15

Luntha la Kulenga​—Mphatso Yochokera kwa Mulungu, 2/1

Maimonides​—Munthu Amene Anamveketsanso Chiyuda, 3/1

Mantha​—Bwenzi Kapena Mdani? 10/15

Mantha​—Ofala Tsopano Koma Osati Kwamuyaya! 10/15

Milungu Yachikazi ya Kubala ndi ya Nkhondo, 11/15

Moyo Wabwino Kwambiri Posachedwapa! 11/15

Moyo Watsopano wa Makolo Athu Akufa, 5/15

Munthu Wanjiru, 9/15

Mwambo Wopanda Tanthauzo? (Kuulula Machimo), 9/15

Njira ya ku Ufulu, 9/1

Nsanje, 9/15

Nsanje Inatsala Pang’ono Kuwononga Moyo Wanga, 9/15

Nthaŵi Zabwinopo Mtsogolo, 8/1

Olamulira Okhala m’Malo a Mizimu, 7/15

Pamene Mwambo Uwombana ndi Choonadi, 12/1

Pamene Sikudzakhalanso Mmphaŵi, 5/1

Phiri Limene “Limayenda,” (Ireland), 4/15

William Tyndale​—Munthu Woona Patali, 11/15

Wosindikiza Amene Anasiya Chizindikiro Chake (Robert Estienne), 4/15

Zaka Makumi Asanu za Kuyesayesa Kosaphula Kanthu (United Nations), 10/1

OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA

1/1, 2/1, 3/1, 4/1, 5/1, 7/1, 8/1, 9/1, 11/1, 12/1

YEHOVA

Ndalama Zimene Zili ndi Dzina la Mulungu, 5/15

YESU KRISTU

Kodi Kukayikira za Yesu Kuli Koyenera? 8/15

Zozizwitsa za Yesu, 3/1

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena