Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w98 12/15 tsamba 31
  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1998

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1998
  • Nsanja ya Olonda—1998
  • Timitu
  • ANACHITA CHIFUNIRO CHA YEHOVA
  • BAIBULO
  • MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA
  • MBONI ZA YEHOVA
  • MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU
  • NKHANI ZA MOYO WA ANTHU
  • NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA
  • YEHOVA
  • YESU KRISTU
Nsanja ya Olonda—1998
w98 12/15 tsamba 31

Zisonyezero za Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1998

Zosonyeza deti la kope lopezekamo nkhaniyo

ANACHITA CHIFUNIRO CHA YEHOVA

Eliya Atamanda Mulungu Woona, 1/1

Paulo Achitira Umboni Molimba Mtima, 9/1

Msamariya Mnansi Wabwino, 7/1

Yesu Anacheza ndi Ana, 11/1

Yesu Atumiza Ophunzira 70, 3/1

Yobu Afupidwa Chifukwa Chokhulupirika, 5/1

BAIBULO

“Baibulo la Chala Chimodzi,” 3/15

Baibulo Latsopano m’Chigiriki Chamakono, 9/1

“Interlinear ya Chipangano Chatsopano Yabwino Koposa,” 2/1

Katswiri wa Maphunziro Asintha Deti la Malembo a Pamanja, 12/15

Kodi Mungalikhulupirire Baibulo? 10/15

Matembenuzidwe a Baibulo Amene Anasintha Dziko Lapansi (Septuagint), 9/15

MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA

Atumwi alephera kuchiritsa mnyamata (Mat. 17:20; Marko 9:29), 8/1

Kukumbukira masiku a ukwati, masiku akubadwa, 10/15

Luka 13:24, 6/15

MBONI ZA YEHOVA

Agamula Kuti Munthu Azidzisankhira (Japan), 12/15

Akapolo a Anthu Kapena Atumiki a Mulungu? 3/15

Baibulo Latsopano m’Chigiriki Chamakono, 9/1

Bolosha la Buku la Anthu Onse, 4/1

“Chitsanzo cha Umodzi ndi Ubale,” 7/15

Chochitika Chosaiŵalika ku France, 7/1

“Gwiritsitsani Chimene Muli Nacho” (Greece), 9/1

Kufikira Ochulukirapo ndi Uthenga Wabwino, 2/15

Kumaliza Maphunziro a Gileadi, 6/1, 12/1

Kuteteza Uthenga Wabwino Mwalamulo, 12/1

Madokotala, Oweruza, ndi Mboni za Yehova, 3/1

Mitima Yonga Mwala Imvetsera (Poland), 10/15

“Mulungu Akonda Wopereka Mokondwera” (zopereka), 11/1

Msonkhano Wachigawo wa “Njira ya Moyo ya Mulungu,” 2/15, 6/1

Nsanjika za Mumzinda Kumka ku Chipululu cha Tundra (Canada), 4/15

Ntchito ‘Yoyeneradi Kulemekezedwa’ (Italy), 8/15

Ntchito Zachikristu Pakati pa Chipwirikiti, 1/15

Pafupi ndi Volokano (Mexico), 8/15

Ukwati Wapadera Kwambiri (Mozambique), 6/15

MOYO NDI MIKHALIDWE YACHIKRISTU

Alemekezeni, 4/1

Chenjerani ndi Chisimoni! 11/15

Ikani Zinthu Zofunika Pamalo Oyamba! 9/1

Luso la Kukopa, 5/15

Khalani ndi Moyo Wopindulitsa, 8/15

Kukonzeratu Tsogolo la Okondedwa Athu, 1/15

Kukwaniritsa Udindo wa Kusamalira Banja, 6/1

Kutengapo Phunziro pa Zolakwa Zakale, 7/1

Kuthetsa Mavuto Mwamtendere, 11/1

Kuyamikira Mwayi wa Utumiki Wopatulika, 8/1

Kuyamikira, 2/15

Makolo Tetezerani Ana Anu! 2/15

Malowolo, 9/15

Miyambo ya Maliro, 7/15

Miyambo ya m’Madera ndi Mapulinsipulo Achikristu, 10/1

“Mtima Womvera,” 7/15

Mungapite Patsogolo Mwauzimu, 5/15

Nchitamando Kapena Kusyasyalika? 2/1

Ndipemphe Ngongole kwa Mbale? 11/15

Pitanibe Patsogolo Mwauzimu! 10/1

Tetezerani Ana Anu, 7/15

Mumayamikira Madalitso a Yehova? 1/1

NKHANI ZA MOYO WA ANTHU

Chachikulu Chimene Ndimafuna Ndicho Kukondweretsa Yehova (T. Neros), 11/1

“Chifundo Chanu Chiposa Moyo” (C. H. Holmes), 2/1

Kulibe Chinthu Chabwino Choposa Choonadi (G. N. Van der Bijl), 1/1

Kusintha Gawo la Utumiki Pausinkhu wa Zaka 80 (G. Matthews), 5/1

Kusiya Kulambira Mfumu ndi Kuyamba Kulambira Koona (I. Sugiura), 12/1

Kuyamikira Choloŵa Cholimba Chachikristu (G. Gooch), 3/1

Ndinachirimika Paziyeso Zoopsa (É. Josefsson), 6/1

Ndinapeza Chinthu Choposa Golidi (C. Mylton), 10/1

Ndinaphunzira Kudalira Yehova (J. Korpa-Ondo), 9/1

Moyo Wanga Monga Wakhate (I. Adagbona), 4/1

“Tangochita Zimene Tayenera Kuzichita” (G. Couch), 8/1

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRA

“Akufa Adzaukitsidwa,” 7/1

Anadedwa Chifukwa cha Chikhulupiriro Chawo, 12/1

Apereka Chiweruzo m’Chigwa Chotsirizira Mlandu, 5/1

Buku la Anthu Onse, 4/1

Buku Lochokera kwa Mulungu, 4/1

Chenjerani ndi Kusakhulupirira, 7/15

Chikhulupiriro Chachikristu Chidzayesedwa, 5/15

Chikhulupiriro ndi Mtsogolo Mwanu, 4/15

Chipulumutso ncha Yehova, 12/15

Gulu la Yehova Limachirikiza Utumiki Wanu, 6/15

Gwiranibe Ntchito Yake ya Chipulumutso Chanu! 11/1

Khalani Otetezereka m’Gulu Lolinganizidwa la Mulungu, 9/1

Khalanibe m’Teokrase, 9/1

Kodi ‘Adzapulumuka Ndani’? 5/1

Kodi Chikhulupiriro Chanu cha Chiukiriro Ncholimba Motani? 7/1

Kodi Mumalidziŵa Bwino Gulu la Yehova? 6/15

Kodi Mwaloŵa Mpumulo wa Mulungu? 7/15

Kodi Ntchito Yanu Idzapulumuka Moto? 11/1

Kukhala Mogwirizana ndi Kudzipatulira Kwachikristu mu Ufulu, 3/15

Kulimbitsa Chidaliro Chathu mwa Chilungamo cha Mulungu, 8/15

Kupatulidwa ndi Ufulu wa Kusankha, 3/15

Kutchinjiriza Chikhulupiriro Chathu, 12/1

Kuyamikira Misonkhano Yachikristu, 3/1

“Kuyembekezera Mwachidwi” 9/15

‘Kuyenda mwa Chikhulupiriro Osati mwa Chionekedwe,’ 1/15

Kuyenda ndi Mulungu​—Masitepe Oyambirira, 11/15

Kuyenda ndi Mulungu​—Tikumadikira Umuyaya, 11/15

Lino Ndilo Tsiku la Chipulumutso! 12/15

Madalitso Aakulu Kudzera m’Pangano Latsopano, 2/1

Madyerero Osaiŵalika a m’Mbiri ya Israyeli, 3/1

“Mtima Wako Ngwowongoka Kodi?” 1/1

Mtundu wa Chikhulupiriro Chanu Ukuyesedwa Tsopano, 5/15

“Mulimbanetu Chifukwa cha Chikhulupiriro”! 6/1

Musaleme Kuthamanga Makani a Moyo! 1/1

Nkhosa Zina ndi Pangano Latsopano, 2/1

Nthaŵi ndi Nyengo Zili m’Manja mwa Yehova, 9/15

‘Pitirizani Kuyenda Mogwirizana ndi Kristu,’ 6/1

Pitirizani Kuyenda ndi Mulungu, 1/15

Tiyenera Kudalira Yehova, 8/15

Tsanzirani Yehova​—Chitani Chilungamo, 8/1

Tsanzirani Chifundo cha Yehova, 10/1

Tsiku la Yehova Layandikira, 5/1

Ufulu Waulemerero Posachedwapa kwa Ana a Mulungu, 2/15

Yehova Atenga Ana Ambiri Aloŵe Ulemerero, 2/15

Yehova Akwaniritsa Malonjezo Ake kwa Okhulupirika, 4/15

Yehova​—Gwero la Chilungamo Chenicheni, 8/1

Yerusalemu​—Kodi Ndiye ‘Woposa Chimwemwe Chanu Chopambana’? 10/15

“Yehova, Mulungu Wachifundo ndi Wachisomo,” 10/1

Yehova ndi Mulungu Wamapangano, 2/1

Yerusalemu​—“Mzinda wa Mfumu Yaikulukulu,” 10/15

Yerusalemu Woyenereradi Dzina Lake, 10/15

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Agora​—Pachimake pa Atene Wakale, 7/15

Akusiyiranji Chipembedzo? 7/1

Amakabe, 11/15

Anapanga Zonsezi Ndani? 5/1

Anthu “Akumva Zomwezi Tizimva Ife” 3/1

Atcheru ndi Zochitika za m’Nthaŵi Yathu? 9/15

Atsogoleri Achipembedzo Amakhulupirira Zimene Amaphunzitsa? 10/15

Ayuganoti, 8/15

Banja​—Lili Pangozi! 4/1

Barnaba​—“Mwana wa Chitonthozo,” 4/15

Beteli​—Mzinda wa Zabwino ndi Zoipa, 9/1

Bwanamkubwa Wonyada (Belisazara), 9/15

Chenjerani ndi Onyoza! 6/1

Chikumbumtima Chanu Mungachikhulupirire? 9/1

Chilungamo Chenicheni​—Liti Ndipo Motani? 6/15

Chilungamo kwa Onse, 8/1

Chisalungamo Sichidzatha? 8/1

Chuma Chingakupatseni Chimwemwe? 5/15

“Choonadi Chidzakumasulani,” 10/1

Choonadi Chimasanduliza Miyoyo, 1/1

Constantine Wamkulu, 3/15

Dariyo, 11/15

Dikirani Moleza Mtima, 6/1

Dziko Lapansi​—Kodi Linakhaliraponji? 6/15

Dziko Lapansi Lidzawonongedwa? 6/15

Filemoni ndi Onesimo, 1/15

Khirisimasi Yanyalanyaza Kristu? 12/15

Kodi Tidzafunikira Magulu Ankhondo Nthaŵi Zonse? 4/15

Kulambira Mulungu m’Choonadi, 10/1

Kusadalirana, 8/15

Kusiyanitsa Chabwino ndi Choipa? 9/1

Mariya Anafa Imfa Yachibadwa? 8/1

Mmene Angelo Angakuthandizireni, 11/15

Mphatso Yachikoka​—Kodi Munthu Atamandidwe Kapena Mulungu Alemekezedwe? 2/15

Ndinu Woyembekezera Zabwino Kapena Zoipa? 2/1

Pamene Mbala Zamfuti Zikuloŵerani, 12/15

‘Pangani Ophunzira mwa Anthu a Mitundu Yonse,’ 1/1

Sanadzipangire Dzina, 3/15

Talmud, 5/15

Tito, 11/15

Tsogolo Lathu Linalembedweratu? 4/15

Tukiko, 7/15

Yunike ndi Loisi, 5/15

Zipembedzo Zikupepesa, 3/1

OLENGEZA UFUMU AKUSIMBA

2/1, 3/1, 4/1, 6/1, 7/1, 8/1, 10/1, 11/1

YEHOVA

Ali Weniweni kwa Inu? 9/15

Kodi Yehova Ndani? 5/1

YESU KRISTU

Kubadwa Kwake, 12/15

Masiku Omaliza Padziko, 3/15

Maziko a Chikhulupiriro Chenicheni, 12/1

Wolamulira Yemwe “Matulukiro Ake Ndiwo Akale Lomwe,” 6/15

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena