Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w13 6/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2013
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2013
w13 6/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

June 15, 2013

© 2013 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino n’ngwathu.

MAGAZINI YOPHUNZIRA

AUGUST 5-11, 2013

Makhalidwe a Yehova Ndi Amtengo Wapatali

TSAMBA 7 • NYIMBO: 69, 89

AUGUST 12-18, 2013

Yehova Ndi Wowolowa Manja Ndiponso Wololera

TSAMBA 12 • NYIMBO: 22, 110

AUGUST 19-25, 2013

Yehova Ndi Wokhulupirika Ndiponso Amakhululuka

TSAMBA 17 • NYIMBO: 63, 77

AUGUST 26, 2013–SEPTEMBER 1, 2013

Lolani Kuti Yehova Azikuumbani ndi Malangizo Ake

TSAMBA 24 • NYIMBO: 120, 64

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Makhalidwe a Yehova Ndi Amtengo Wapatali

▪ Yehova Ndi Wowolowa Manja Ndiponso Wololera

▪ Yehova Ndi Wokhulupirika Ndiponso Amakhululuka

Akhristufe timadziwa kuti Yehova ali ndi makhalidwe akuluakulu anayi. Koma nkhani zitatuzi zitithandiza kuona kuti makhalidwe enanso a Yehova amene sitikambiranakambirana ndi amtengo wapatali kwambiri. Tikambirana mmene Yehova amasonyezera khalidwe lililonse ndiponso zimene tingachite kuti timutsanzire.

▪ Lolani Kuti Yehova Azikuumbani ndi Malangizo Ake

Pofotokoza mphamvu imene Yehova ali nayo pa anthufe, Malemba amanena kuti iye ali ngati “Wotiumba.” (Yes. 64:8) Nkhaniyi ikusonyeza kuti tingaphunzire zambiri zokhudza Yehova poona mmene iye ankaumbira anthu m’mbuyomo. Ikufotokozanso mmene iye amatithandizira akamatiumba masiku ano.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

3 Ndadalitsidwa Kwambiri Chifukwa Chomvera Yehova

22 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

29 Akulu, Kodi Mumalimbikitsa Anthu ‘Olefuka’?

32 Kodi Mukukumbukira?

PATSAMBA LOYAMBA: Akulalikira mumsewu mumzinda wa Frankfurt ku Germany

GERMANY

KULI ANTHU

81,751,600

KULI MBONI

162,705

MAPHUNZIRO A BAIBULO

74,466

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO

265,407

[Chithunzi patsamba 2]

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena