Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w14 10/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2014
  • Timitu
  • MAGAZINI YOPHUNZIRA
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2014
w14 10/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

October 15, 2014

© 2014 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MAGAZINI YOPHUNZIRA

DECEMBER 1-7, 2014

Tizikhulupirira Kwambiri Ufumu wa Mulungu

TSAMBA 7 • NYIMBO: 108, 129

DECEMBER 8-14, 2014

‘Mudzakhala Ufumu wa Ansembe’

TSAMBA 13 • NYIMBO: 98, 102

DECEMBER 15-21, 2014

Kodi Mumayamikira Mwayi Wogwira Ntchito ndi Yehova?

TSAMBA 23 • NYIMBO: 120, 44

DECEMBER 22-28, 2014

“Ikani Maganizo Anu pa Zinthu Zakumwamba”

TSAMBA 28 • NYIMBO: 70, 57

NKHANI ZOPHUNZIRA

▪ Tizikhulupirira Kwambiri Ufumu wa Mulungu

▪ ‘Mudzakhala Ufumu wa Ansembe’

Mulungu akugwiritsa ntchito Ufumu wa Mesiya pokwaniritsa cholinga chake padzikoli. M’nkhanizi tiona mapangano angapo amene akukhudza Ufumuwu komanso zifukwa zotichititsa kuukhulupirira kwambiri.

▪ Kodi Mumayamikira Mwayi Wogwira Ntchito ndi Yehova?

Nkhaniyi ikufotokoza za atumiki a Yehova akale komanso a masiku ano. Itithandiza kuti tiziyamikira kwambiri mwayi wogwira ntchito ndi Mulungu.

▪ “Ikani Maganizo Anu pa Zinthu Zakumwamba”

M’masiku otsiriza ano, pali zinthu zambiri zimene zingasokoneze chikhulupiriro chathu. Panalinso zinthu zimene zikanasokoneza chikhulupiriro cha Abulahamu ndi Mose. Kodi tikuphunzira chiyani kwa anthu awiriwa? Nkhaniyi itithandiza kuti tipirire chifukwa itilimbikitsa kuganizira kwambiri za Yehova Mulungu ndi Ufumu wake.

M’MAGAZINIYI MULINSO NKHANI IZI

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse ku Taiwan

18 Zinthu Zosaiwalika pa Utumiki Wanga

PATSAMBA LOYAMBA: Alongo awiri akulalikira mumsewu pafupi ndi mapiri enaake, m’tauni ya Tausa kudera la Taita

KENYA

KULI ANTHU

44,250,000

KULI OFALITSA

26,060

MAPHUNZIRO A BAIBULO

43,034

OPEZEKA PA CHIKUMBUTSO MU 2013

60,166

[Chithunzi patsamba 2]

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena