Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w17 May tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
w17 May tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

MLUNGU WA JULY 3-9, 2017

3 Tizithandiza Alendo Kuti ‘Azitumikira Yehova Mokondwera’

MLUNGU WA JULY 10-16, 2017

8 Kodi Tingathandize Bwanji Ana a Anthu Ochokera M’mayiko Ena?

Nkhani yoyamba ikufotokoza mavuto amene abale ndi alongo omwe athawa kwawo amakumana nawo komanso zimene tingachite powathandiza. Nkhani yachiwiri ikufotokoza mmene mfundo za m’Baibulo zingathandizire anthu amene asamukira m’dziko lina kuti azisankha zinthu mwanzeru pothandiza ana awo.

13 Mbiri ya Moyo Wanga​—Vuto Losamva Silinandilepheretse Kuphunzitsa Anthu Ena Baibulo

MLUNGU WA JULY 17-23, 2017

17 Musalole Kuti Chikondi Chanu Chizirale

MLUNGU WA JULY 24-30, 2017

22 “Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?”

Kukhala m’dziko loipali si kophweka. Koma nkhanizi zikusonyeza mmene tingapewere mtima wodzikonda wa m’dzikoli tikamapitiriza kukonda Yehova, choonadi ndiponso abale ndi alongo athu. Zikufotokozanso zimene tingachite kuti tizikonda kwambiri Khristu m’malo mokonda zinthu za m’dzikoli.

27 Kodi Gayo Ankathandiza Bwanji Akhristu Anzake?

30 Moyo Wosalira Zambiri Ndi Wosangalatsa

31 Kale Lathu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena