Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/94
  • Zilengezo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zilengezo
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1994
Utumiki Wathu wa Ufumu—1994
km 3/94

Zilengezo

◼ Mabuku ogwiritsira ntchito mu March: Mafunso Achichepere Akufunsa—Mayankho Amene Amathandiza. April ndi May: Sabusikripishoni ya Nsanja ya Olonda. June: Mafunso Achichepere Akufunsa—Mayankho Amene Amathandiza. CHIDZIŴITSO: Mipingo imene idzafuna zinthu za mkupiti zotchulidwazo iyenera kuziodetsa pa fomu yawo yotsatira ya mwezi ndi mwezi ya Literature Order (S-14).

◼ Kuyambira mlungu wa June 13, 1994, buku la Kupangitsa Moyo Wanu wa Banja Kukhala Wachimwemwe lidzaphunziridwa pa Phunziro Labuku Lampingo m’Chicheŵa.

◼ Aliyense wogwirizana ndi mpingo ayenera kutumiza masabusikripishoni atsopano ndi akulembetsanso onse a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani!, kuphatikizapo masabusikripishoni aumwini, kupyolera mumpingo.

◼ Woyang’anira wotsogoza kapena munthu wina wogaŵiridwa ndi iye ayenera kuŵerengera maakaunti ampingo pa March 1 kapena mwamsanga pambuyo pake. Lengezani kumpingo mutachita zimenezi.

◼ Mabuku Omwe Alipo:

Chingelezi: 1994—Yearbook of Jehovah’s Witnesses.

◼ Mabuku Omwe Mulibe m’Sitoko Kwachikhalire:

Chicheŵa: Mitu ya Nkhani ya Baibulo Yokambitsirana. Chingelezi: Mitu ya Nkhani ya Baibulo Yokambitsirana.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena