Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/09 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 15

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 15
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 15
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 6/09 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa June 15

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 15

Nyimbo Na. 175

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 21 ndime 1-8

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Levitiko 6-9

Na. 1: Levitiko 8:1-17

Na. 2: ‘Kodi Mumakhulupirira za Machiritso?’ (rs-CN tsa. 170 ndime 3 ndi 4)

Na. 3: Chifukwa Chake Tiyenera Kupewa Bodza (lr-CN mutu 22)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 25

Mph.5: Zilengezo.

Mph.10: Lalikirani Uthenga Wabwino. Nkhani yolimbikitsa yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, patsamba 279, ndime 1 mpaka 4.

Mph.10: Ngati Wina Anena Kuti, ‘Ndimakhulupirira Chisinthiko.’ Kukambirana ndi omvera kuchokera m’buku la Kukambitsirana, patsamba 104 ndi 105. Phatikizanipo chitsanzo chachidule chosonyeza mmene tingayankhire ngati wina akunena kuti, ‘Ndimakhulupirira kuti Mulungu analenga munthu kupyolera mwa chisinthiko.’

Mph.10: “Konzekerani Bwino Pokaphunzitsa.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 68

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena