Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/09 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 24

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 24
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 24
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 8/09 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa August 24

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 24

Nyimbo Na. 38

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl-CN mutu 24, ndime 11-21, ndi bokosi, tsa. 249

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Numeri 14-16

Na. 1: Numeri 14:26-43

Na. 2: Kodi Kukonda Chilamulo cha Mulungu Kumatanthauza Chiyani? (Sal. 119:97)

Na. 3: Amene Angatitonthoze (lr-CN mutu 31)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 218

Mph.5: Zilengezo.

Mph.10: Konzekerani Kugawira Nsanja ya Olonda ya September 1 ndi Galamukani! ya September. Fotokozani mwachidule zimene zili m’magaziniwo. Pemphani omvera kuti atchule funso limene angafunse kuti ayambitse makambirano komanso lemba limene angawerenge asanagawire magaziniwo. Chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri zosonyeza mmene tingagawirire magaziniwa.

Mph.20: “Zimene Tingachite Kuti Tizilalikira kwa Amuna Ambiri.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho. Mukakambirana ndime 9, funsani mkulu mmodzi kuti afotokoze chimene chinamuthandiza kuyesetsa kuti apeze mwayi wa utumiki mumpingo. Kodi waphunzitsidwa zotani ndipo anaphunzitsidwa ndi ndani?

Nyimbo Na. 204

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena