Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/10 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 25

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 25
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 25
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 1/10 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa January 25

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 25

Nyimbo Na. 27

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 2, ndime 12-21 ndi bokosi patsamba 24a

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Oweruza 5-7

Na. 1: Oweruza 7:1-11

Na. 2: Kodi Tingamudziwe Bwanji “Mkazi Wachiwerewere Wamkulu” Wotchulidwa pa Chivumbulutso 17:1?

Na. 3: Kodi Pali Munthu Aliyense Amene Anayamba Watuluka mu Helo Wotchulidwa M’Baibulo? (rs tsa. 145 ndime 5.)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 12

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Mabuku Ogawira mu February. Fotokozani mwachidule mfundo zikuluzikulu za m’buku limene tidzagawire mu February. Chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa akuchita ulaliki wamwamwayi n’kugawira bukulo ndiponso kuyambitsa phunziro la Baibulo.

Mph. 20: “Kodi Mumanyalanyaza?” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Ikambidwe ndi mkulu. Chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa akufotokozera dokotala ntchito ya khadi la DPA ndi kumupempha kuti alisunge m’faelo ya wofalitsayo. Dokotalayo akulonjeza kuti adzatero. Pomaliza, werengani ndime yomaliza.

Nyimbo Na. 29

[Mawu a M’munsi]

a Mungasankhe kukambirana bokosi kapena ayi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena