Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/10 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 1

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 1
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 1
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 1/10 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa February 1

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 1

Nyimbo Na. 26

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 3, ndime 1-7 ndi bokosi patsamba 29

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Oweruza 8-10

Na. 1: Oweruza 8:1-12

Na. 2: Kodi Pali Chilango Chamuyaya Kaamba ka Oipa? (rs tsa. 146 ndime 3 mpaka tsa. 147 ndime 2)

Na. 3: Kodi Kudziwa Zimene Zimachitika Munthu Akamwalira N’kothandiza Bwanji?

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 54

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Zosowa za Pampingo.

Mph. 10: Kuyambitsa Maphunziro a Baibulo. Tchulani tsiku loyambitsa maphunziro a Baibulo. Tchulani zinthu zosangalatsa zimene zinachitika mu utumiki wakumunda. Apo ayi funsani woyang’anira utumiki kapena wofalitsa waluso kuti afotokoze njira yoyambitsira maphunziro a Baibulo yothandiza kwambiri m’dera lanu. Mwina mungamupemphe kuti achite chitsanzo cha zimene zinachitika.

Mph. 10: Gwiritsani Ntchito Zinthu Zooneka mu Utumiki. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki patsamba 247 ndime 1 mpaka 248 ndime 1.

Nyimbo Na. 44

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena