Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/10 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 8
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 8
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 2/10 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa February 8

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 8

Nyimbo Na. 23

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 3 ndime 8-15, ndi bokosi la patsamba 30a

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Oweruza 11–14

Na. 1: Oweruza 13:1-14

Na. 2: Kodi Tikuphunzira Chiyani pa Mawu a Yesu Opezeka pa Luka 16:9-13?

Na. 3: Kodi Mawu a M’buku la Chivumbulutso Akuti ‘Kuzunzidwa kwa Muyaya’ Amatanthauza Chiyani? (rs tsa. 147 ndime 3 ndi 4)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 40

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kuyankha Mafunso Okhudza Maholide. Kukambirana ndi omvera kuchokera m’buku la Kukambitsirana, kuyambira patsamba 241 ndime 4 mpaka tsamba 243 ndime 2. Kodi anthu a m’dera lanu amakonda kuchita zikondwerero ziti? Kodi ndi malo ati kumene mungalalikire panthawi ya chikondwerero chinachake? Chitani chitsanzo chosonyeza kholo likuthandiza mwana wake mmene angayankhire ngati atafunsidwa kuti, ‘N’chifukwa chiyani sukondwerera Isitala?’

Mph. 20: “Kugawira Timapepala Toitanira Anthu ku Chikumbutso.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho. Musanakambirane ndime 2, gawirani aliyense kapepala koitanira anthu ku Chikumbutso, ngati muli nato, ndipo fotokozani mbali zosiyanasiyana za kapepalako. Mukamaliza kukambirana ndime 2, wofalitsa achite chitsanzo chosonyeza mmene angagawirire kapepalaka. Funsani woyang’anira utumiki kapena mkulu wina kuti afotokoze zimene mpingo wakonza panthawi yogawira timapepalati.

Nyimbo Na. 18

a [Mawu a M’munsi]

Mungasankhe kukambirana bokosi kapena ayi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena