Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/10 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 22

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 22
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 22
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 2/10 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa February 22

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 22

Nyimbo Na. 34

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv Zakumapeto  tsamba 207-209

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Oweruza 19-21

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 20

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Buku Logawira mu March. Funsani ofalitsa awiri kuti anene zinthu zimene aona kuti n’zothandiza m’bukuli ndiponso maulaliki ogwira mtima amene akhala akuwagwiritsa ntchito pogawira bukuli m’gawo lanu. Aliyense achite chitsanzo kapena ayerekezere zimene anachita pogwiritsa ntchito bukuli poyambitsa phunziro la Baibulo.

Mph. 10: Kuphunzitsa M’njira Yokambirana Kumalimbikitsa Anthu Kumvetsera. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 251 mpaka tsamba 253, ndime 1.

Mph. 10: Tsogolerani Anthu Achidwi ku Gulu la Yehova. Kambiranani ndi omvera ndime zitatu kuyambira pakamutu ka patsamba 99 m’buku la Gulu. Funsani omvera kuti afotokoze zimene anachita potsogolera anthu achidwi ku gulu la Yehova. Funsani wofalitsa amene wapindula chifukwa chakuti amene ankamuphunzitsa Baibulo anamutsogolera kugulu la Yehova.

Nyimbo Na. 31

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena