Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/10 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa March 29

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa March 29
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 29
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 3/10 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa March 29

MLUNGU WOYAMBIRA MARCH 29

Nyimbo Na. 45

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 5 ndime 1-6 ndi mabokosi a patsamba 52 ndi 55

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Samueli 14-15

Na. 1: 1 Samueli 14:​24-35

Na. 2: Njira Zimene Tingayandikirire kwa Yehova (Yak. 4:⁠8)

Na. 3: Kodi Anzeru a Kummawa, Kapena Kuti Amagi, Amene Nyenyezi Inawatsogolera kwa Yesu Anali Ndani? (rs tsa. 240 ndime 2-4)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 2

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kuyambitsa Maphunziro a Baibulo. Lengezani tsiku lotsatira loyambitsa maphunziro a Baibulo. Funsani wofalitsa amene anakwanitsa kuyambitsa maphunziro a Baibulo panthawi imeneyi ndipo akuwachititsabe. Ndi nkhani ziti zimene iye waona kuti zikugwira mtima anthu a m’gawolo ndipo zikuthandiza kuyambitsa maphunziro? Kodi iye saiwala mfundo iti pochita maulendo obwereza? M’pempheni kuti achite chitsanzo pankhani imodzi mwa nkhani zimene iye waona kuti zikuthandiza kuyambitsa maphunziro a Baibulo.

Mph. 10: Bokosi la Mafunso. Ikambidwe ndi mkulu woyenera.

Mph. 10: “Muzithandizana mu Utumiki.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 39

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena