Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/10 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 12
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 12
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 4/10 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa April 12

MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 12

Nyimbo Na. 16

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 5 ndime 16-23

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Samueli 19-22

Na. 1: 1 Samueli 21:1-9

Na. 2: Kodi Tiyenera Kuona Motani Zinthu Zimene Yehova Amadana Nazo? (Miy. 6:16-19)

Na. 3: Kodi Tiyenera Kutsatira Mfundo Ziti pa Nkhani ya Zikondwerero Zilizonse? (rs tsa. 241 ndime 4–tsa. 242 ndime 3)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 9

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Afikeni Omvera Anu Pamtima Mwa Kuwalimbikitsa Kulingalira. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, kuyambira patsamba 58 ndime 3, mpaka kumapeto kwa kamutu patsamba 59.

Mph. 20: “Kopani Chidwi Pophunzitsa.” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho. Mukatha kukambirana ndime 4, pemphani mpainiya kuti achite chitsanzo cha mmene tingayambire phunziro la Baibulo pogwiritsa ntchito buku lakuti Baibulo Limaphunzitsa Chiyani ndipo agwiritse ntchito mfundo za m’nkhani ino.

Nyimbo Na. 10

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena