Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/10 tsamba 6
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 31

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 31
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 31
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 5/10 tsamba 6

Ndandanda ya Mlungu wa May 31

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 31

Nyimbo Na. 37

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 7 ndime 20-28

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Samueli 16-18

Na. 1: 2 Samueli 17:1-13

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Yesu Amatchedwa “Mbuye wa Sabata”? (Mat.12:8)

Na. 3: Kodi Tiyenera Kulambira “Oyera Mtima” Monga Otiimira kwa Mulungu? (rs tsa. 435 ndime 9–tsa. 436 ndime 4)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 35

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: “Kodi Munayamba Mwasonyezapo Munthu pa Ulendo Woyamba Mmene Timachitira Phunziro la Baibulo?” Nkhani. Fotokozani maganizo amene ali mu nkhaniyo ndipo kenako chitani chitsanzo chosonyeza mmene mungawagwiritsire ntchito.

Mph. 20: “Mmene Mungaphunzitsire Ofalitsa Atsopano Kulalikira.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Mukamaliza kukambirana ndime 5, chitani chitsanzo chosonyeza mkulu akulalikira ndi wofalitsa watsopano. Wofalitsa watsopanoyo akulalikira kwa munthu koma sanayese kumuwerengera munthuyo lemba lililonse. Atachoka pakhomo la munthuyo, mkuluyo akumupatsa malangizo mwanzeru komanso mwachikondi. Akumulimbikitsa watsopanoyo kuti azigwiritsa ntchito Baibulo pakhomo lililonse.

Nyimbo Na. 22

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena