Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/10 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 19
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 19
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 7/10 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa July 19

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 19

Nyimbo Na. 24

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 9, ndime 22-26 ndi bokosi patsamba 109; Zakumapeto, kuyambira pakamutu patsamba 218-219a

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mafumu 12-14

Na. 1: 1 Mafumu 12:12-20

Na. 2: Kodi N’chiyani Chingatithandize Kuti Tiziona Abale Athu Mmene Yehova Amawaonera?

Na. 3: Tetezani Ubwenzi Wanu ndi Yehova, Ndipo Pewani Mayanjano Oipa (rs tsa. 172 ndime 2)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 35

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 8: Njira Zowonjezera Utumiki Wanu—Gawo 2. Nkhani yochokera m’buku la Gulu, tsamba 112, ndime 3, mpaka tsamba 114, ndime 1. Funsani mpainiya mmodzi kapena apainiya awiri ndipo afotokoze zimene anasintha pa moyo wawo kuti athe kuchita upainiya.

Mph. 12: “Kugulitsa Malonda pa Misonkhano Yathu Yachigawo.” Kambiranani ndi omvera. Limbikitsani onse kubweretsa chakudya m’malo mochoka pamalo amsonkhano kukagula chakudya kwa amene ayala malonda pamsewu kapena kumalesitilanti.

Mph. 10: “Kodi Ndikuchita Zokwanira?” Kambiranani mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 28

[Mawu a M’munsi]

a Mungasankhe kuwerenga bokosi kapena Zakumepeto.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena