Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/10 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 23

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 23
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 23
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 8/10 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa August 23

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 23

Nyimbo Na. 44

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 11 ndime 10-19

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mafumu 5-8

Na. 1: 2 Mafumu 6:8-19

Na. 2: Kodi N’chifukwa Chiyani Mabaibulo Ambiri Sagwiritsa Ntchito Dzina Lenileni la Mulungu Kapena Limangopezeka Nthawi Zochepa? (rs tsa. 417 ndime 9 mpaka tsa. 418 ndime 4)

Na. 3: Kodi Zingatheke Bwanji Kuti Chilakolako cha Thupi Chikhale Mulungu? (Afil. 3:18, 19)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 52

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Yambitsani Phunziro la Baibulo pa Ulendo Woyamba mu September. Nkhani yokambirana ndi omvera. M’mwezi wa September tidzagawira buku la Baibulo Limaphunzitsa Chiyani. Tidzayesetse kukambirana ndime imodzi kapena ziwiri ndi mwininyumba pa ulendo woyamba. Kambiranani njira zingapo zimene mungachitire zimenezi. Khalani ndi chitsanzo chimodzi kapena ziwiri zosonyeza njira zimenezi.

Mph. 20: “Mukhoza Kukwanitsa Kulalikira Mwamwayi.”—Gawo 1. Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Kambiranani ndime 1 mpaka 8. Khalani ndi chitsanzo chimodzi kapena ziwiri zosonyeza mmene tingagwiritsire ntchito mfundo za m’nkhaniyi polalikira mwamwayi.

Nyimbo Na. 31

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena