Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/10 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 30

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 30
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 30
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 8/10 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa August 30

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 30

Nyimbo Na. 44

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 11 ndime 10-19

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mafumu 9-11

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 49

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: “Kodi Mwagwiritsapo Ntchito Tsamba Lomaliza?” Nkhani yokambirana ndi omvera. Pogwiritsa ntchito mfundo zimene zili mu nkhaniyi, khalani ndi chitsanzo chosonyeza mmene tingagawire Nsanja ya Olonda ya September 1. Kenako sankhani nkhani imodzi kapena ziwiri za mu Galamukani! ya September ndipo pemphani omvera kuti atchule mafunso ndi malemba amene angagwiritse ntchito pogawira magaziniyi pogwiritsa ntchito nkhani zimenezi. Khalani ndi chitsanzo chosonyeza mmene tingagawire Galamukani! imeneyi.

Mph. 20: “Mukhoza Kukwanitsa Kulalikira Mwamwayi.”—Gawo 2. Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Kambiranani ndime 9 mpaka 13 ndi bokosi la patsamba 6.

Nyimbo Na. 31

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena